Yoswa
MUTU1
1NdipokunaliatafaMosemtumikiwaYehova,Yehova ananenandiYoswamwanawaNuni,mtumikiwaMose, ndikuti,
2Mosemtumikiwangawafa;tsononyamuka,nuoloke Yordanouyu,iwendianthuawaonse,kulowam’dziko limenendiwapatsaanaaIsrayeli.
3Maloonseamenemapazianuadzapondapondakupatsani inu,mongandinanenakwaMose
+4KuyambirakuchipululundikuLebanoni+mpaka kumtsinjewaukulu,mtsinjewaFirate,+dzikolonsela Ahiti,+mpakakuNyanjaYaikuluyakuloweradzuwa,+ ndiyemalireanu.
5Palibemunthuadzaimapamasopakomasikuonsea moyowako;mongandinakhalandiMose,momwemo ndidzakhalandiiwe;sindidzakusiya,sindidzakutaya.
6Khalawamphamvu,nulimbikemtima,pakutiudzagawira anthuawadzikolo,limenendinalumbiriramakoloaokuti ndidzawapatsa,likhalecolowacao.
7Komakhalawamphamvundiwolimbamtimandithu, kutiusamalirekuchitamongamwachilamulochonse chimeneMosemtumikiwangaanakulamulirani;
8Bukuililachilamulolisachokepakamwapako;koma uzilingiriramousanandiusiku,kutiusamalirekuchita mongamwazonsezolembedwamo;
9Kodisindinakulamuliraiwe?Khalawamphamvu, limbikamtima;usaope,kapenakutengankhawa,pakuti YehovaMulunguwakoalindiiwekulikonseumukako.
10PamenepoYoswaanalamuliraakapitawoaanthu,kuti, 11Pitapakatipakhamulo,nuuzeanthu,ndikuti, Konzekeraniinuzakudya;+pakutipasanathemasikuatatu mudzawolokaYorodanoameneyukutimulowem’dziko limeneYehovaMulunguwanuakupatsanikutilikhalelanu lanu.
12NdipoYoswaananenakwaArubeni,ndiAgadi,ndi hafuyafukolaManase,kuti, 13KumbukiranimawuameneMosemtumikiwaYehova anakulamulirani,kuti,YehovaMulunguwanu wakupumulitsani,nakupatsanidzikoili
14Akazianu,anaanuaang’ono,nding’ombezanu adzakhalam’dzikolimeneMoseanakupatsanitsidyalijala Yordano;komainumudzaolokapamasopaabaleanu okonzeka,amunaonseamphamvundiolimbamtima,ndi kuwathandiza;
15kufikiraYehovaatapumulitsaabaleanu,monga anakupatsaniinu,kutiiwonsoalandiredzikolimene YehovaMulunguwanuawapatsa;pamenepo mudzabwererakudzikolanulanu,ndikulidya,limene MosemtumikiwaYehovaanakupatsanitsidyalijala Yordano,kotulukiradzuwa
16NdipoanayankhaYoswa,nati,Zonsemwatilamulira tidzachita,ndikulikonsemudzatitumizaifetidzamuka.
17MongatinamveraMosem’zonse,momwemo tidzamverainu;komaYehovaMulunguwanuakhalendi inu,mongaanalindiMose
+18Aliyensewopandukira+malamuloanu,+osamvera mawuanu+m’zonsezimenemunamulamula,+aziphedwa.
MUTU2
1NdipoYoswamwanawaNunianatumizaamunaawiri okazondamtserikucokerakuShitimu,nati,Mukani, muonedziko,ndiloYerikoNdipoanamuka,nalowa m'nyumbayamkaziwadama,dzinalakeRahabi,nagona kumeneko
2NdipoanauzamfumuyaYeriko,kuti,Taonani,analowa munousikuunoamunaaanaaIsrayelikudzazondadziko. 3NdipomfumuyaYerikoinatumizauthengakwaRahabi, ndikuti,Tulutsaamunaameneafikakwaiwe,amene alowam’nyumbamwako,pakutiabwerakudzazondadziko lonse
4Ndipomkaziyoanatengaamunaawiriaja,nawabisa,nati, Anadzakwaineamuna,komasindinadziwakumene akuchokera;
5Ndipokunali,potsekapacipata,kutada,amunawo anaturuka;kumeneanankaamunawosindikudziŵa;pakuti mudzawapeza
6Komaiyeanawakwerapamwambapatsindwilanyumba, nawabisandimapesiafulakesi,ameneanawayala patsindwi
7NdipoamunawoanawalondolapanjirayakuYorodano yopitakumadooko;
8Ndipoasanagone,iyeanakwerakwaiwopadenga;
9Ndipoiyeanatikwaamunawo,NdidziŵakutiYehova wakupatsanidzikoli,ndikutimanthaanuatigwera,ndikuti onseokhalam’dzikoakomokachifukwachainu
10PakutitinamvakutiYehovaanaphwetsamadzia m’NyanjaYofiirapamasopanu,mujamunatulukamu Igupto;ndizimenemunachitiramafumuawiriaAamori okhalakutsidyalijalaYordano,SihonindiOgi,amene munawaonongakonse
11Ndipotitangomvazimenezi,mitimayathu inasungunuka,+ndipopalibemunthuameneanakhala wolimbamtimachifukwachainu,+pakutiYehova MulunguwanundiyeMulunguwakumwambandipadziko lapansi.
12Tsopano,ndikukupemphani,mulumbirirekwaYehova +kuti,popezandakukomeranimtima,+inunso mudzachitirabanjalaatatewangakukomamtima+ndi kundipatsachizindikirochoona
13ndikutimupulumutseatatewanga,ndiamayiwanga, ndiabaleanga,ndialongoanga,ndizonsealinazo,ndi kupulumutsamoyowathukuimfa
14Ndipoamunawoanamyankhaiye,Moyowathum’malo mwanu,mukapandakunenazantchitoyathuiyi.Ndipo kudzali,pameneYehovawatipatsadzikolo,tidzakucitira cifundondicoonadi
15Pamenepoanawatsitsapazenerandichingwe,pakuti nyumbayakeinalipalingalamudzi,ndipoiyeanakhala pamwambapalinga
16Ndipoiyeanatikwaiwo,Pitaniinukuphiri,kuti olondolaangakumanenanu;ndipomubisalekomweko masikuatatu,mpakaabwerereolondolawo;
17Ndipoamunawoanatikwaiye,Tidzakhalaopanda cholakwapalumbirolakolimenewatilumbiritsa
18Taona,tikadzalowam’dzikolo,uzimangachingwe chofiirachipazeneralimenewatitsitsirapo,ndipoubwere nawokunyumbakwakoatatewako,ndiamako,ndiabale ako,ndionseam’nyumbayaatatewako
19Ndipokudzali,kutialiyenseakaturukapamakomoa nyumbayakokumkakukhwalala,mwaziwakeudzakhala pamutupace,ndipoifetidzakhalaopandamlandu;
20Ndipoukaululanchitoyathuiyi,sitidzakhalaopanda chilumbirochakochimenewatilumbiritsa.
21Ndipoiyeanati,Mongamwamauanu,zikhale chomwechoNdipoiyeanawalolaamuke,ndipoiwo anamuka:namangaiyechingwechofiirapazenera.
22Ndipoanamuka,nafikakuphiri,nakhalakomweko masikuatatu,kufikiraolondolawoanabwerera;ndipo olondolawoanawafunafunapanjirayonse,koma sanawapeza
23Pamenepoamunaaŵiriwoanabwerera,natsika m’phirimo,naoloka,nafikakwaYoswamwanawaNuni, namuuzazonsezinawagwera;
24NdipoanatikwaYoswa,Zoonadi,Yehovawapereka dzikolonsem’manjamwathu;pakutingakhaleonseokhala m’dzikoakomokachifukwachaife
MUTU3
1NdipoYoswaanalawiramamawa;nacokerakuSitimu nafikakuYordano,iyendianaonseaIsrayeli,nagona kumenekoasanaoloke
2Ndipopanaliatapitamasikuatatu,akapitaoanapitapakati pakhamulo;
3Ndipoanauzaanthukuti,Mukawonalikasalapanganola YehovaMulunguwanu,ndiansembeAlevialikulisenza, pamenepomuzicokakwanu,ndikulitsata
4Komapakhaledangapakatipainundiilo,monga mikonozikwiziwirindimuyeso;musayandikirepamenepo, kutimudziwenjiraimenemuyenerakupitamo;
5NdipoYoswaanatikwaanthu,Dziyeretseni,pakuti mawaYehovaadzachitazodabwitsapakatipanu.
6Yoswaanauzaansembekuti:“Nyamulanilikasala panganondikupitapatsogolopaanthuwoNdipo ananyamulalikasalacipangano,natsogoleraanthu.
7NdipoYehovaanatikwaYoswa,Lerondidzayamba kukukuzapamasopaAisrayelionse,kutiadziwekuti mongandinakhalandiMose,momwemondidzakhalandi iwe
8Ndipouwauzeansembeakunyamulalikasalacipangano, ndikuti,Mukafikam’mphepetemwamadziaYordano, muimem’Yordano
9YoswaanauzaanaaIsiraelikuti:“Bweranikuno,mumve mawuaYehovaMulunguwanu.
10NdipoYoswaanati,Mwaichimudzadziwakuti Mulunguwamoyoalipakatipanu,ndikutiadzapitikitsa ndithupamasopanuAkanani,ndiAhiti,ndiAhivi,ndi Aperizi,ndiAgirigasi,ndiAamori,ndiAyebusi
11Taonani,likasalapanganolaAmbuyewadzikolonse lapansilikuolokapamasopanukulowaYordano.
12Tsopanodzitengereniamunakhumindiaŵirimwa mafukoaIsrayeli,pafukolirilonsemwamunammodzi
13Ndipokudzali,pamenemapaziaansembeakunyamula likasalaYehova,Ambuyewadzikolonselapansi, akakhazikikam’madziaYordano,madziaYordano adzadulidwam’madziotsikakuchokerakumwamba;ndipo adzaimapamulu
14Ndiyenoanthuatachokam’mahemaawokutiawoloke Yorodano,ansembeonyamulalikasalachipangano+ pamasopaanthu
+15OnyamulaLikasawoatafikakuYorodano,+mapazia ansembeonyamulalikasawoanalikumizidwam’mphepete mwamadzi,+chifukwamtsinjewaYorodanounali kusefukiram’mphepetemwanyanjayonsenthawiyokolola. 16kutimadziotsikapamwambaanaima,nakwerapamulu patalindithukuchokerakumudziwaAdamu,umeneuli pafupindiZaretani:ndiotsikirakunyanjayaChigwa, ndiyoNyanjayamchere,anaphwa,nadulidwa:ndipoanthu anaolokapandunjipaYeriko
17AnsembeonyamulalikasalapanganolaYehovaanaima molimbapanthakayoumapakatipamtsinjewaYorodano, ndipoAisiraelionseanaolokapoumampakaanthuonse anawolokaYorodano.
MUTU4
1Ndipokunali,pameneanthuonseanaolokaYordano, YehovaananenandiYoswa,ndikuti, 2Mudzitengereamunakhumindiawirimwaanthu, mwamunammodzipafukolililonse;
3Ndipomuwauze,ndikuti,Chotsaniinupanopakatipa Yordano,pamalopamenemapaziaansembeanaima olimba,miyalakhumindiiwiri,nimunyamukenayo pamodzindiinu,ndikuisiyam’nyumbayaalendo,mmene mugonausikuuno.
4PamenepoYoswaanaitanaamunakhumindiaŵiri, ameneanawasankhamwaanaaIsrayeli,pafukolirilonse mwamunammodzi.
5Yoswaanawauzakuti:“Wolokanipatsogolopalikasala YehovaMulunguwanundikulowapakatipamtsinjewa Yorodano,+ndipoaliyensewainuanyamulemwala paphewapake,+mongamwakuwerengakwamafukoa anaaIsiraeli
6Kutiicicikhalecizindikilomwainu,kutipameneana anuadzafunsamakoloaom’tsogolo,ndikuti,Mwalauwu mukutanthauzaciani?
7Pamenepomuwayankhekuti,MadziaYordano anadulidwapamasopalikasalapanganolaYehova; poolokaYordano,madziaYordanoanadulidwa;ndipo miyalaiyiikhalechikumbutsokwaanaaIsrayelikosatha. 8NdipoanaaIsrayelianachitamongaYoswa adawalamulira,natolamiyalakhumindiiwiripakatipa Yordano,mongaYehovaadauzaYoswa,mongamwa kuwerengakwamafukoaanaaIsraele,naolokanayo kumalokumeneadagona,naiikapamenepo
9Yoswaanaimikamiyala12pakatipamtsinjewa Yorodano,pamalopameneanaimamapaziaansembe onyamulalikasalachipangano,ndipoilipompakalero.
10Ansembeonyamulalikasaanaimapakatipamtsinjewa Yorodano,mpakaanamalizazonsezimeneYehovaanauza Yoswakutianenekwaanthu,mongamwazonseMose analamulaYoswa.
11Ndipokunali,pameneanthuonseanaoloka,kutilikasa laYehovalinaoloka,ndiansembe,pamasopaanthu 12NdipoanaaRubeni,ndianaaGadi,ndihafuyafukola Manase,anaolokandizidazankhondopamasopaanaa Israyeli,mongaMoseadawauza.
13Pafupifupianthu40,000okonzekerankhondo anawolokapamasopaYehovakupitakunkhondo m’zidikhazaYeriko.
14TsikulimeneloYehovaanakulitsaYoswapamasopa Aisrayelionse;ndipoanamuopaiyemongaanaopaMose masikuonseamoyowake
15NdipoYehovaananenandiYoswa,nati, +16Lamulaansembeameneakunyamulalikasalamboni +kutiatulukemuYorodano
17PamenepoYoswaanalamuliraansembe,ndikuti, Kweranimutulukem’Yordano.
18Ndipokunali,ansembeakunyamulalikasalacipangano laYehovaatakwerakuturukapakatipaYordano,ndi kukwezekamapaziaansembekumkakumtunda,madzia Yordanoanabwereram’malomwao,nasefukiramagombe aceonse,mongaanacitapoyamba.
19Ndipoanthuanatulukam’Yordanopatsikulakhumila mweziwoyamba,namangamsasakuGiligala,kumalirea kum’mawakwaYeriko.
20Ndipomiyalakhumindiiwiriija,imeneanatengamu Yordano,YoswaanaimangakuGiligala
21NdipoanalankhulandianaaIsrayeli,ndikuti,Pamene anaanuadzafunsamakoloaom’tsogolo,kuti,Miyalaiyi nchiyani?
22Pamenepomuzidziwitsaanaanu,ndikuti,Aisrayeli anaolokaYordanouyupamtundawouma
23PakutiYehovaMulunguwanuanaphwetsamadzia Yordanopamasopanu,kufikiramunaoloka,monga YehovaMulunguwanuanachitirapaNyanjaYofiira, imeneanaphwetsapamasopathu,mpakatinaoloka; 24Kutianthuonseapadzikolapansiadziwedzanjala Yehova,kutindilamphamvu,+kutimuziopaYehova Mulunguwanumpakakalekale
MUTU5
1Ndipokunali,pamenemafumuonseaAamoriokhala tsidyalijalaYordanokumadzulo,ndimafumuonsea Akananiokhalam’mbalimwanyanja,anamvakutiYehova anaphwetsamadziaYordanopamasopaanaaIsrayeli, mpakatinaoloka,mitimayaoinasungunuka,ndipo munalibensomzimumwaiwocifukwacaanaaIsrayeli
2PanthawiyoYehovaanauzaYoswakuti:“Udzipangire mipeniyakuthwa,ndipoudulensoanaaIsiraelikachiwiri
3NdipoYoswaanadzipangiramipeniyakuthwa,nadula anaaIsrayelikuphirilakhungu.
4ChifukwachakeYoswaanawadulandiichi:Anthuonse ameneanatulukamuIgupto,amuna,amunaankhondo, anaferam’chipululupanjira,atatulukam’Aigupto.
5Tsopanoanthuonseameneanatulukaanaliodulidwa, komaanthuonseameneanabadwiram’chipululupanjira potulukamuIguputo,sanawadule
6PakutianaaIsrayelianayendam’cipululuzakamakumi anai,mpakaanathaanthuonseankhondo,oturuka m’Aigupto,popezasanamveramauaYehova;
7Anaawoameneanawautsam’malomwawo,amene Yoswaanawadula,+chifukwaanaliosadulidwa+ chifukwasanawadulem’njira
8Ndipokunali,atathakudulaanthuonse,anakhalam’malo mwaom’cigonokufikiraanachira.
9NdipoYehovaanatikwaYoswa,Lerondakucotsanipa inucitonzocaAiguptoCifukwacaceanachadzinalacela malowo,Giligala,kufikiralerolino.
10NdipoanaaIsrayelianamangamisasakuGiligala, nachitapasikapatsikulakhumindichinayilamwezi madzulo,m’zidikhazaYeriko
11Ndipom’mawamwacepambuyopapasika,anadya zipatsozakalezam’dzikolo,mikateyopandacotupitsa,ndi tiriguwokazingatsikulomwelo
12Ndipomanaanalekam’mawamwace,atadyakozipatso zakalezam’dziko;ndipoanaaIsrayelianalibensomana; komaanadyazipatsozadzikolaKananichakachimenecho
13Ndipokunali,pameneYoswaanalipafupindiYeriko, anatukulamasoakenapenya,ndipo,taonani,munthu anaimapopenyanandiiye,ndilupangalakelosolola m’dzanjalake;
14Ndipoiyeanati,Iyayi;komandabweratsopanomonga kazembewakhamulaYehovaNdipoYoswaanagwa nkhopeyakepansi,nalambira,natikwaiye,Mbuyewanga anenanjindikapolowake?
15NdipokazembewakhamulaYehovaanatikwaYoswa, Bvulansapatoyakokumapaziako;pakutimalooyimapo ndiopatulikandipoYoswaanachitachomwecho
MUTU6
1TsopanoYerikounatsekedwakwambirichifukwacha anaaIsiraeli:panalibewotulukakapenakulowa.
2NdipoYehovaanatikwaYoswa,Taona,ndapereka m’manjamwakoYeriko,ndimfumuyake,ndingwazizake 3Ndipomuzizunguliramzindawo,amunanonseankhondo, ndikuzunguliramzindawokamodziMuziteromasiku asanundilimodzi
4Ndipoansembeasanundiawiriazinyamulamalipenga asanundiawirianyangazamphongopamasopalikasa; 5Ndipokudzali,kutiakalizalipengalalitali,ndipo pakumvakulirakwalipenga,anthuonseadzafuulandi kufuulakwakukulu;ndipolingalamzindawolidzagwa pansi,ndipoanthuadzakwera,yensemolunjikapamaso pake.
6YoswamwanawaNunianaitanaansembe+n’kuwauza kuti:“Nyamulanilikasalapangano+ndipoansembe7 azinyamulamalipenga7anyangazankhosa+patsogolopa likasalaYehova
7Ndiyenoanauzaanthuwokuti:“Pitani,kuzungulira mzindawo,ndionyamulazidaatsogolerelikasalaYehova. 8NdiyenoYoswaatalankhulandianthu,ansembe7 onyamulamalipenga7anyangazankhosa+anapita pamasopaYehovandikulizamalipengawo,+ndipolikasa lapanganolaYehovalinawatsatira
9Anthuonyamulazidawoanapitapatsogolopaansembe ameneanalikuimbamalipenga,+ndipoenaanatsatira Likasa,ndipoansembewoanalikuyenda+ndikuliza malipengawo
10Yoswaanalamulaanthuwokuti:“Musafuule,kapena kufuula,kapenamawualionseasatulukepakamwapanu mpakatsikulimenendidzakuuzanikutifuulanipamenepo mudzafuula
11NdipolikasalaYehovalinazunguliramudzi, kuuzungulirakamodzi;
12Yoswaanadzukam’mamawa,ndipoansembe ananyamulalikasalaYehova
13Ansembeasanundiaŵirionyamulamalipenga7 anyangazankhosa+patsogolopalikasalaYehova anapitirizabekuyendandikulizamalipengawokoma
Yoswa
otsalirawoanatsatalikasalaYehova,ansembeakuyendabe ndikulizamalipenga.
14Ndipotsikulachiwirianazunguliramzindawokamodzi, nabwererakumsasa;anateromasikuasanundilimodzi.
15Ndipokunali,tsikulacisanundiciwiri,iwoanalawira mamawa,m’bandakucha,nazunguliramudzimonga momwemokasanundikawiri; 16Ndipokunalipanthawiyacisanundiciwiri,ansembe analizamalipenga,Yoswaananenandianthu,Fuulani; pakutiYehovawakupatsanimudziwo
17Ndipomudziwoudzakhalawotembereredwakwa Yehova,iwowondizonsezirim’mwemo; 18Ndipoinu,dzipangenikonsekuchinthuchoperekedwa choperekedwacho,mungadzitengereotembereredwa, pakutengakochinthuchoperekedwacho,ndikuchititsa msasawaIsraelekukhalatemberero,ndikuusokoneza. 19Komasilivayense,golide,ndiziwiyazamkuwandi zachitsulo,zikhalazopatulikirakwaYehova; 20Pamenepoanthuanapfuula,ansembeanalizamalipenga; ndipokunachitika,pameneanthuanamvakulirakwa lipenga,ndipoanthuanapfuulandikufuulakwakukuru, ndipolingalinagwapansi,ndianthuanakwerakumka kumudzi,yensepolunjikapamasopake,nalandamzindawo 21Ndipoanawonongandilupangazonsezam’mudzi, amunandiakazi,anandiakulu,nding’ombe,ndinkhosa, ndiabulu,ndilupangalakuthwa
22KomaYoswaanauzaamunaawiriajaanakazonda dzikolokuti:“Lowanim’nyumbayamkaziwachigololoyo, mutulutsemomkaziyondizonsealinazo,monga munalumbirirakwaiye
23Ndipoanyamataameneazondianalowa,naturutsa Rahabi,ndiatatewace,ndiamace,ndiabaleace,ndizonse analinazo;naturutsaabaleaceonse,nawasiyakunjakwa cigonocaIsrayeli.
24Ndipoanatenthamzindawondimotondizonsezinali m’mwemo;
25NdipoYoswaanalekaRahabiwadamayo,ndibanjala atatewake,ndizonseanalinazo;ndipoanakhalam’Israyeli kufikiralerolino;popezaanabisaamithengaameneYoswa anawatumakutiakazondeYeriko.
26NdipoYoswaanawalumbiritsapanthawiyo,kuti, AtembereredwepamasopaYehovamunthuamene adzaukandikumangamudziuwuwaYeriko;
27ChoteroYehovaanalindiYoswa;ndipombiriyake inamvekam’dzikolonselo
MUTU7
1KomaanaaIsrayelianalakwirachoperekedwacho;pakuti Akani,mwanawaKarimi,mwanawaZabidi,mwanawa Zera,wafukolaYuda,anatengakochoperekedwacho; ndipomkwiyowaYehovaunayakiraanaaIsraele.
2NdipoYoswaanatumizaamunaakuYerikokuAi, umeneulipafupindiBetaveni,kum’maŵakwaBeteli, nanenanao,nati,KweranimukawonedzikoNdipo amunawoanakweranapenyaAi
3NdipoanabwererakwaYoswa,nanenanaye,Asakwere anthuonse;komaakwereamunangatizikwiziwirikapena zitatu,nakantheAi;osakakamizaanthuonsekugwira ntchitokumeneko;pakutialiowerengeka.
4Pamenepoanakwerakoamunangatizikwizitatu;
5NdipoamunaakuAianaphaamunangatimakumiatatu mphambuasanundimmodzi,popezaanawathamangitsa kuyambirakuchipatakufikirakuSebarimu,nawakantha potsikirapo;chifukwachakemitimayaanthuinasungunuka, nikhalamadzi.
6NdipoYoswaanang’ambazovalazake,nagwankhope yakepansipamasopalikasalaYehovakufikiramadzulo, iyendiakuluaIsrayeli,nathirafumbipamutupawo.
+7Yoswaanati:“Kalangaine,+Yehova,Ambuye WamkuluKoposa,+n’chifukwachiyanimwawoloka anthuwaYorodanokutiatiperekem’manjamwaAamori kutiatiwononge?Mwenzitikadakhalaokondwakukhala tsidyalijalaYordano!
8OAmbuye,ndidzanenachiyanipameneIsrayeli atembenuziraadaniawokumbuyo?
9PakutiAkananindionseokhalam’dzikoadzamva, nadzatizinga,ndikuchotsadzinalathupadzikolapansi; 10NdipoYehovaanatikwaYoswa,Nyamuka;wagonanji pamasopako?
+11Aisiraeliachimwa,+ndipoaphwanyapangano+ limenendinawalamulira,+pakutiatengansochinthu choperekedwachoperekedwacho,akuba,akunyengerera,+ n’kuchiikapakatipakatunduwawo
12ChonchoanaaIsiraelisanathekuimapamasopaadani awo,+komaanatembenukiram’mbuyo+pamasopaadani awo,+chifukwaanaliotembereredwa
13Nyamuka,patulaanthuwo,nunenekuti,Mudzipatulire mawa,pakutiateroYehovaMulunguwaIsrayeli,Pali choperekedwachotembereredwapakatipanu,Israyeli;
14Cifukwacacem’mawamudzakutengeranimongamwa mafukoanu;ndibanjalimeneYehovaadzalitenga lidzabwerandimabanjaawo;ndiponyumbaimeneYehova adzaitengaidzabweramunthundimunthu
15Ndipokudzali,kutiiyeamenewagwidwandichinthu choperekedwachoperekedwayo,atenthedwendimoto,iye ndizonsealinazo;
16ChoteroYoswaanadzukam’mamawan’kubweretsa AisiraelimongamwamafukoawondipofukolaYuda linasankhidwa;
17NdipoanabweretsabanjalaYuda;natengabanjala Azera,natengerabanjalaAzeramwamunammodzi;ndipo Zabdianatengedwa
18Ndipoanalowam’nyumbamwakemunthundimunthu; ndipoAkani,mwanawaKarimi,mwanawaZabidi, mwanawaZera,wafukolaYuda,anasankhidwa
19YoswaanauzaAkanikuti:“Mwanawanga,patsa YehovaMulunguwaIsiraeliulemerero,+ndipouulule kwaiye.ndiuzetsopanochimenewachita;usandibisire.
20NdipoAkanianayankhaYoswa,nati,Zoonadi ndinachimwiraYehovaMulunguwaIsrayeli,ndipo ndachitazakutizakuti;
21Pamenendinaonamwazofunkhachovalachokongola chakuBabulo,ndimasekeliasilivamazanaawiri,ndi mphakowagolidiwolemeramasekelimakumiasanu, ndinazikhumba,ndikuzitenga;ndipotaonani,zabisika pansipakatipahemawanga,ndisilivapansipake
22PamenepoYoswaanatumizaamithenga,nathamangira kuhemako;ndipotaonani,zobisikam'hemawake,ndi silivapansipake
23Ndipoanazitulutsam’chihemacho,nabweranazokwa Yoswa,ndikwaanaonseaIsraele,naziikapamasopa Yehova
24NdipoYoswa,ndiAisrayelionsepamodzinaye, anatengaAkanimwanawaZera,ndisiliva,ndichobvala, ndimpheteyagolidi,ndianaakeaamuna,ndianaaakazi, nding’ombezake,ndiabuluake,ndinkhosazake,ndi hemawake,ndizonseanalinazo,ndipoanapitanazo kuchigwachaAkori
25NdipoYoswaanati,Wativutitsanji?Yehova adzakuvutitsanilero.NdipoAisrayelionseanamponya miyala,nawatenthandimoto,atawaponyamiyala
26Ndipoanaunjikamuluwaukuluwamiyalapamwamba pake,kufikiralerolino+ChonchoYehovaanasintha mkwiyowakewaukaliCifukwacaceanachadzinalacela malowo,ChigwachaAkori,kufikiralerolino.
MUTU8
1NdipoYehovaanatikwaYoswa,Usaope,usaopsedwa; tengaankhondoonsenawe,nukwere,nukwerekuAi;taona, ndaikam'dzanjalakomfumuyaAi,ndianthuake,ndi mudziwake,ndidzikolace;
2NdipouchitireAindimfumuyakemongaunachitira Yerikondimfumuyake;zofunkhazakezokha,ndi ng’ombezake,muzilandenokha;ikaniolaliramzindawo kumbuyokwake
3PamenepoYoswaananyamuka,ndianthuonseankhondo, kutiakwerekukamenyanandiAi;
4Ndipoanawauza,kuti,Taonani,mubisaliramzindawo, kuserikwamzindawo;
5Ndipoine,ndianthuonseokhalandiine,tidzayandikira kumudzi;
6(Pakutiadzatulukapambuyopathu)kufikiratitawakokera kumudzi;pakutiadzati,Athawapamasopathumonga poyambapaja;chifukwachaketidzathawapamasopawo
7Pamenepomuzinyamukapobisalira,ndikulanda mzindawo,pakutiYehovaMulunguwanuadzaupereka m’manjamwanu
8Ndipokudzali,mutalandamzindawo,muzitenthetsa mudziwo;muzichitamongamwalamulolaYehova Taonani,ndakulamulirani
9ChonchoYoswaanawatumiza,ndipoiwoanapita kukabisalira+n’kukakhalapakatipaBetelindiAi,+ kumadzulokwaAi,+komaYoswaanagonausiku umenewopakatipaanthuwo.
10NdipoYoswaanadzukam’mamawa,nawerengaanthu, nakwera,iyendiakuluaIsrayeli,patsogolopaanthukuAi 11Ndipoanthuonse,ndiwoankhondoameneanalinaye, anakwera,nayandikira,nafikapamasopamzindawo, namangamahemaaokumpotokwaAi;pakatipawondiAi panalichigwa
12Ndipoanatengaamunangatizikwizisanu,nawabisalira pakatipaBetelindiAi,kumadzulokwamzindawo 13Ataikaanthuwo,khamulonselankhondolimenelinali kumpotokwamzindawo,ndiolalirakumadzulokwa mzinda,+usikuumenewoYoswaanalowapakatipa chigwacho
14MfumuyaAiitangoonazimenezi,inafulumirakudzuka m’mawakwambiri,ndipoamunaamumzindawoanatuluka kukamenyanandiAisiraeli,iyendianthuakeonse,pa nthawiyoikidwiratukuchigwakomasanadziwakuti alalirakuserikwamzindawo.
15NdipoYoswandiAisrayelionseanachitangati agonjetsedwapamasopawo,nathawanjirayakuchipululu
16PamenepoanthuonseameneanalikuAianasonkhana kutiawathamangitse,ndipoanathamangitsaYoswa, nakokedwakutalindimzindawo
+17Palibemunthuameneanatsalam’AikapenakuBeteli amenesanatulukekuthamangiraIsiraeli,+ndipoanasiya mzindauliwotseguka+ndikuthamangitsaAisiraeli
18NdipoYehovaanatikwaYoswa,Lozamkondouli m’dzanjalakokuAi;pakutindidzauperekam’dzanjalako. NdipoYoswaanatambasuliramkondoumeneanalinawo m’dzanjalakekumzindawo
19Ndipoolalirawoananyamukamsangam’malomwao, nathamangaatangotambasuladzanjalake,nalowam’mudzi, naulanda,nafulumirakuutenthamzindawo.
20NdipoamunaakuAiatacheuka,anapenya,ndipo taonani,utsiwamzindawoukukwerakumwamba,ndipo analibemphamvuyothawirakwinakapenakwina; 21YoswandiAisrayelionseataonakutiolaliraalanda mzindawo,ndikutiutsiwamzindawoukukwera, anatembenukanaphaamunaakuAi.
22Ndipoenaanaturukam’mudzikukamenyananao; nakhalapakatipaIsrayeli,enambaliiyi,enambaliina;
23NdipomfumuyaAianaigwirayamoyo,nabweranayo kwaYoswa
24Ndipokunali,atathaIsrayelikuphaonseokhalam’Ai kuthengo,m’cipululucimeneanawapirikitsa,nagwaonse ndilupangalakuthwa,kufikiraanatha,Aisrayelionse anabwererakuAi,naukanthandilupangalakuthwa
25Ndipokunaterokutionseameneanagwatsikulimenelo, amunandiakazi,ndiwozikwikhumindiziwiri,ndiwo amunaonseakuAi
26PakutiYoswasanabwezedzanjalakem’mbuyolimene anatambasulanalomkondo,kufikiraataonongakonse anthuonseakuAi
27Komang’ombendizofunkhazamudziwoAisrayeli anadzifunkha,mongamwamauaYehovaamene analamuliraYoswa
28YoswaanatenthamzindawaAi+n’kuusandutsabwinja mpakakalekale,ngakhalebwinjampakalero
29NdipomfumuyaAianaipachikapamtengokufikira madzulo;ndipolitaloŵadzuŵa,Yoswaanalamulirakuti atsitsemtembowakepamtengo,nauponyepolowerapa chipatachamudzi,naunjikepomuluwawukuluwamiyala, umeneudakalipompakalero.
30PamenepoYoswaanamangiraYehovaMulunguwa Israyeliguwalansembem’phirilaEbala;
31MongaMosemtumikiwaYehovaanalamuliraanaa Israyeli,mongamwalembedwam’bukulachilamulocha Mose,guwalansembelamiyalayamphumphu,lopanda munthuasanyamulepochitsulo;
32Ndipoanalembapamenepopamiyalakopiyachilamulo chaMose,chimeneanachilembapamasopaanaaIsrayeli 33NdipoAisrayelionse,ndiakuluao,ndiakapitao,ndi oweruzaao,anaimirirambaliiyindimbaliyaLikasa, pamasopaansembeAlevionyamulalikasalacipanganola Yehova,ndimlendo,ndiwobadwapakatipao;hafuyaiwo moyang’anizanandiphirilaGerizimu,ndihafuyaiwo moyang’anizanandiphirilaEbala;mongaMosemtumiki waYehovaadalamulirakale,kutiadalitseanaaIsraele 34Pambuyopakeanawerengamawuonseachilamulo, madalitsondimatemberero,mongamwazonse zolembedwam’bukulachilamulo
35PanalibemawuamodzipazonsezimeneMose analamulira,ameneYoswasanawawerengepamasopa khamulonselaIsiraeli,+akazindianaaang’onondi alendoogonerapakatipawo.
MUTU9
1Ndipokunali,pamenemafumuonseokhalakutsidyalina laYordano,kumapiri,ndim’zigwa,ndim’zigawozonseza NyanjaYaikulupandunjipaLebanoni,Ahiti,ndiAamori, Akanani,Aperizi,Ahivi,ndiAyebusi,anamva; 2IwoanasonkhanapamodzikutiamenyanendiYoswandi Isiraelindimtimaumodzi.
3AnthuakuGibeoniatamvazimeneYoswaanachitira YerikondiAi
4Anachitamwanzeru,namuka,nadzipangangati akazembe,natengamatumbaakalepaabuluawo,ndi matumbaavinyoakale,ong’ambika,ndiomanga;
5Ndinsapatozakale,ndizopindikapamapaziawo,ndi zobvalazakale;ndimkatewonsewambutozaounali woumandiwankhungu
6NdipoanapitakwaYoswakumsasakuGiligala,nanena nayendikwaamunaaIsrayeli,Tachokerakudzikolakutali;
7NdipoamunaaIsrayelianatikwaAhivi,Kapena mukukhalapakatipathu;ndipotidzapanganananubwanji?
8NdipoanatikwaYoswa,NdifeakapoloanuNdipo Yoswaanatikwaiwo,Ndinuyani?ndipomuchokerakuti?
9Ndipoanatikwaiye,Akapoloanuachokerakudziko lakutalindithu,chifukwachadzinalaYehovaMulungu wanu;
10NdizonsezimeneanachitiramafumuawiriaAamori ameneanalikutsidyalinalaYorodano,Sihonimfumuya Hesiboni,ndiOgimfumuyaBasana,ameneanaliku Asitaroti.
11Cifukwacaceakuluathundinzikazonsezam’dziko lathuananenandiife,ndikuti,Tenganizakudyaza paulendo,mupitekukakomananao,ndikunenanao,Ndife akapoloanu;
12Mkatewathuuwutinautengawamotom’nyumbazathu, ukhalembutowathu,tsikulimenetinatulukakudzakwa inu;komatsopano,taonani,yauma,ndiyankhungu; 13Ndipomabotoloawaavinyo,tidadzaza,analiatsopano; ndipo,taonani,zang’ambika:ndizobvalazathuizi,ndi nsapatozathuzakalambachifukwachaulendowautali ndithu
14Ndipoamunawoanatengakocakudyacao,osafunsira uphungupakamwapaYehova
15NdipoYoswaanapangananaomtendere,napangananao panganolakuwalekandimoyo;
16Ndipokunali,pakuthakwamasikuatatuatapangananao pangano,anamvakutianalianansiao,ndikutianali kukhalapakatipao.
17NdipoanaaIsrayelianayendaulendo,nafikakumidzi yaotsikulachitatuTsopanomidziyawoinaliGibeoni,ndi Kefira,ndiBeeroti,ndiKiriyati-yearimu
18NdipoanaaIsrayelisanawakantha,popezaakalongaa khamuadawalumbiriramwaYehovaMulunguwaIsrayeli. Ndipokhamulonselinadandaulamotsutsanandiakalonga 19Komaakalongaonseanatikwakhamulonse,Ife tawalumbirirapaYehovaMulunguwaIsrayeli;
20Izitidzawachitira;tidzawasiyaamoyo,kutikapena mkwiyoungatigwerechifukwachalumbirolimene tinawalumbirira
21Ndipoakalongaanatikwaiwo,Alekeniakhalendi moyo;komaakhaleotemankhuni,ndiotungiramadzia khamulonse;mongaakalongaanawalonjeza
22NdipoYoswaanawaitana,nanenanao,kuti, Mwatinyengabwanji,ndikuti,Takhalakutalindithundi inu;mukakhalapakatipathu?
23Cifukwacacendinuotembereredwa,ndipopalibewa inuameneadzalekakukhalakapolo,otemankhuni,ndi otungiramadzianyumbayaMulunguwanga
24NdipoanayankhaYoswa,nati,Popezaanauzidwa ndithuatumikianu,kutiYehovaMulunguwanu analamuliramtumikiwakeMose,kukupatsanidziko lonselo,ndikuonongaokhalam’dzikolopamasopanu, chifukwachaketinaopakwambirimoyowathuchifukwa chainu,ndipotachitaichi
25Ndipotsopano,taonani,tilim’dzanjalanu;
26Ndipoanawachitiramomwemo,nawalanditsam’dzanja laanaaIsrayeli,kutiasawaphe
27TsikulomweloYoswaanawapangakukhalaotema nkhunindiotungiramadziamsonkhanondiguwa lansembelaYehova,mpakalero,pamaloameneiye adzasankhe.
MUTU10
1Ndipokunali,pameneAdonizedekimfumuya YerusalemuanamvakutiYoswaanalandaAi,nauononga konse;mongaanachitiraYerikondimfumuyake, momwemoanachitiraAindimfumuyake;ndikutiokhala m’GibeonianacitamtenderendiIsrayeli,nakhalapakati pao;
2Iwoanachitamanthakwambiri+chifukwaGibeoniunali mzindawaukulungatiumodziwamizindayachifumu,+ ndiponsochifukwachakutiunaliwaukulukuposaAi,+ndi amunaakeonseamphamvu
3ChonchoAdonizedekimfumuyakuYerusalemu anatumizauthengakwaHohamumfumuyakuHeburoni, ndikwaPiramumfumuyakuYarimuti,ndikwaYafiya mfumuyakuLakisi,ndikwaDebirimfumuyakuEgiloni 4Kweranikwaine,ndikundithandiza,kutitikanthe Gibeoni,chifukwaiwoanapanganamtenderendiYoswa ndianaaIsiraeli
5ChoteromafumuasanuaAamori,mfumuyaYerusalemu, mfumuyaHebroni,mfumuyaYarimuti,mfumuyaLakisi, mfumuyakuEgiloni,anasonkhanapamodzi,nakwera,iwo ndimakamuawoonse,namangamisasapamasopa Gibeoni,namenyananawo
6NdipoamunaakuGibeonianatumizauthengakwa YoswakumisasakuGiligala,ndikuti,Musalekereredzanja lanukwaanyamataanu;+13mukwererekwaifemsanga, +mutipulumutse+ndikutithandiza,+pakutimafumuonse aAamoriokhalakumapiriatisonkhanirakutiatiwukire
7PamenepoYoswaanakwerakuchokerakuGiligala,iye ndianthuonseankhondopamodzinaye,ndingwazizonse.
8NdipoYehovaanatikwaYoswa,Usawaopa,pakuti ndawaperekam’dzanjalako;palibemmodziwaiwo adzaimapamasopanu.
9ChonchoYoswaanawafikiramodzidzimutsa,+ndipo anakwerausikuwonsekuchokerakuGiligala
10NdipoYehovaanawakanthapamasopaAisrayeli, nawaphamakanthidweaakulukuGibeoni,nawapirikitsa panjirayokwerakuBetihoroni,nawakanthakufikiraku Azeka,ndikuMakeda.
11Ndipokunali,pameneanalikuthawapamasopa Aisrayeli,alipotsikirakuBetihoroni,Yehova anawagwetseramiyalaikuluikuluyocokerakumwambapa iwo,kufikirakuAzeka,nafa:ameneanafandimatalala anacurukaiwoameneanaaIsrayelianawaphandilupanga 12PamenepoYoswaananenandiYehovatsikulija YehovaanaperekaAamoripamasopaanaaIsrayeli,nati pamasopaIsrayeli,Dzuwa,imaniiwepaGibeoni;ndiiwe, Mwezi,m’chigwachaAjaloni.
13Ndipodzuwalinaima,ndimweziunakhala,kufikira anthuatabwezerachilangoadaniawoKodiizi sizinalembedwem'bukulaYaseri?Tsonodzuwalinaima pakatipathambo,silinafulumirekulowatsikulathunthu 14Ndipopanalibetsikulotere,lisanafikeilokapena pambuyopake,kutiYehovaanamveramawuamunthu, pakutiYehovaanamenyerankhondoIsrayeli
15PamenepoYoswandiAisrayelionsepamodzinaye anabwererakumsasakuGiligala.
16Komamafumuasanuwaanathawa,nabisalam’phanga lakuMakeda
17NdipoanamuuzaYoswa,kuti,Mafumuasanuaja apezedwaobisikam’phangalakuMakeda
18NdipoYoswaanati,Kunkhuniziranimiyalaikuluikulu pakamwapaphanga,nimuikepoamunaakuwasunga;
19Ndipomusaime,komathamangitsaniadanianu,ndi kukanthaam’mbuyomwawo;musawalolekulowa m’midzimwao,pakutiYehovaMulunguwanu wawaperekam’dzanjalanu
20NdiyenoYoswandianaaIsiraeliatangomaliza kuwaphandikuwaphandikuwapha,+mpakakuwathera,+ ndipootsalawoanalowam’mizindayokhalandimipanda yolimbakwambiri
21NdipoanthuonseanabwererakumsasakwaYoswaku Makedandimtendere;
22PamenepoYoswaanati,Tsegulanipakamwapaphanga, ninditulutsirem’phangamafumuasanuajakwaine.
23Ndipoanachitachomwecho,namturutsam’phanga mafumuasanuwo,mfumuyaYerusalemu,mfumuyaku Hebroni,mfumuyakuYarimuti,mfumuyakuLakisi,ndi mfumuyakuEgiloni
24Ndipokunali,atatulutsamafumuwokwaYoswa,Yoswa anaitanaamunaonseaIsrayeli,natikwaakapitaoa ankhondoameneanamukanaye,Senderani,muikemapazi anupamakosiamafumuawa.Ndipoanayandikira,naika mapaziawopamakosiawo
25NdipoYoswaanatikwaiwo,Musaope,kapenakutenga nkhawa,limbikani,mulimbemtima;
26PambuyopakeYoswaanawakantha,nawapha, nawapachikapamitengoisanu;
27Ndipokunali,pakuloŵadzuŵa,Yoswaanalamulira, ndipoanawatsitsam’mitengo,naziponyam’phanga m’meneanabisika,naikamiyalaikuluikulum’kamwamwa phanga,imeneilipokufikiralerolomwe.
28YoswaanalandamzindawaMakedatsikulomwelo+ n’kukanthandilupangalakuthwa,+motimfumuya kumenekoanaiwonongandianthuonseameneanali mmenemo+IyeanachitiramfumuyaMakeda+monga mmeneanachitiramfumuyakuYeriko
29PamenepoYoswandiAisiraelionseameneanalinaye anachokakuMakedan’kupitakuLibinan’kuyamba kumenyanandimzindawaLibina
30Yehovaanaperekansomzindawundimfumuyake m’manjamwaIsiraeli.ndipoanaukanthandilupanga lakuthwa,ndiamoyoonseanalim'mwemo;asasiyemondi mmodziyense;komaanacitakwamfumuyacemonga anacitiramfumuyaYeriko.
31YoswandiAisiraelionseameneanalinayeanachokaku Libinan’kupitakuLakisi,n’kumangamsasapafupindi mzindawon’kuuthirankhondo
32YehovaanaperekaLakisim’manjamwaIsiraeli,+ ameneanaulandatsikulachiwiri,+n’kuunthandilupanga lakuthwa,+ndianthuonseameneanalimmenemo, mogwirizanandizonsezimeneanachitakuLibina
33PamenepoHoramumfumuyakuGezerianakwera kudzathandizaLakisi;ndipoYoswaanamkanthaiyendi anthuace,kufikirasanamsiyirandimmodziyense
34NdipoYoswaanacokerakuLakisi,ndiAisrayelionse pamodzinayekumkakuEgiloni;ndipoanauzinga,nauthira nkhondo;
35Ndipoanaulandatsikulomwelo,naukanthandilupanga lakuthwa,naonongakonseamoyoonseanalim’mwemo tsikulomwelo,mongamwazonseanachitiraLakisi
36NdipoYoswaanakwerakuchokerakuEgiloni,ndi Aisrayelionsepamodzinaye,kunkakuHeburoni;ndipo adamenyananawo
37Anaulandandikuuphandilupangalakuthwa,ndi mfumuyake,ndimizindayakeyonse,ndianthuonse ameneanalimmenemo;sanasiyendimmodziyense, mongamwazonseanachitiraEgiloni;komaanauononga konse,ndiamoyoonseanalim’mwemo
38PamenepoYoswandiAisrayelionsepamodzinaye anabwererakuDebiri;nalimbananawo;
39Ndipoanaulanda,ndimfumuyake,ndimidziyake yonse;ndipoanawakanthandilupangalakuthwa,naononga konseamoyoonseanalim'mwemo;sanasiyandimmodzi yense;mongaanachitiraHebroni,momwemoanachitira Debirindimfumuyake;mongansoanachitiraLibinandi mfumuyake.
40ChoteroYoswaanakanthadzikolonselakumapiri,+la kumwera,+lakuchigwa,+lakuakasupe,+ndimafumu awoonse,+motisanasiyendimmodziyemwe,+koma anawonongazonsezamoyo+mongammeneYehova MulunguwaIsiraelianalamulira
41NdipoYoswaanawakanthakuyambirakuKadesibarineakufikirakuGaza,ndidzikolonselaGoseni, kufikirakuGibeoni.
42MafumuonsewandidzikolawoYoswaanawalanda nthawiimodzi,chifukwaYehovaMulunguwaIsiraeli anamenyerankhondoIsiraeli
43NdipoYoswaanabwerera,ndiAisrayelionsepamodzi naye,kumsasakuGiligala
MUTU11
1Ndipokunali,pameneYabinimfumuyakuHazori anamvazimenezo,anatumizakwaYobabumfumuya Madoni,ndikwamfumuyakuSimironi,ndikwamfumu yaAkasafu;
2ndimafumuokhalakumpotokwamapiri,ndikuzigwa kummwerakwaKineroti,ndikuchigwa,ndimalireaDori kumadzulo;
3ndiAkananikum’maŵa,ndikumadzulo,ndikwaAamori, ndiAhiti,ndiAperizi,ndiAyebusikumapiri,ndikwa AhivikunsikwaHermoni,m’dzikolaMizipa
4Ndipoanatuluka,iwondimakamuawoonsepamodzi nao,anthuambiri,mongamchengawam’mphepetemwa nyanja,ndiakavalondimagaretaambirindithu
5Mafumuonsewaatasonkhanapamodzi,anadzanamanga misasapamodzipamadziaMeromu,kutiamenyanendi Israyeli
6NdipoYehovaanatikwaYoswa,Usawaopa,pakuti mawanthawiinondidzawaperekaonseophedwapamaso paAisrayeli;
7ChoteroYoswandianthuonseankhondoameneanali nayeanafikamodzidzimutsakudzakumananawokumadzi aMeromundipoadawagwera
8Yehovaanawaperekam’manjamwaIsiraeli,+amene anawakantha+ndikuwathamangitsa+mpakakuZidoni+ waukulu,+mpakakuMisirefoti-maimu+ndimpaka kuchigwachaMizipa+kum’mawa.ndipoanawakantha, mpakasanawasiyirendimmodziyense
9NdipoYoswaanawachitiramongaYehovaadamuuza;
10Yoswaanabwereram’mbuyopanthawiyon’kukalanda mzindawaHazori+n’kuphamfumuyakendilupanga chifukwamzindawaHazoriunalilikululamaufumu onsewopoyamba.
11Iwoanaphaanthuonseameneanalimmenemondi lupangalakuthwa,+n’kuwawonongeratu,+motipanalibe wopumawopuma,+motianatenthamzindawaHazorindi moto
12Ndipomidziyonseyamafumuaja,ndimafumuawo onse,Yoswaanalanda,nawakanthandilupangalakuthwa, nawaonongakonse,mongaanalamuliraMosemtumikiwa Yehova
13Komamidziimeneinaimam’zitundazawo,Isiraeli sanaitenthe,kupatulapoHazoriwokha;zomweYoswa anaziwotcha
14Zofunkhazonsezamidziiyinding’ombeanaaIsrayeli anadzifunkha;komaanakanthamunthualiyensendi lupangalakuthwa,kufikiraadawaononga,osasiyaaliyense wakupuma.
15MongaYehovaanalamuliraMosemtumikiwake, momwemoMoseanalamuliraYoswa;sanasiyakanthu kalikonsepazonseYehovaadalamuliraMose.
16ChoteroYoswaanalandadzikolonselo,lamapiri,+ dzikolonselakumwera,+dzikolonselaGoseni,+ lachigwa,+lachigwa,+lamapiriaIsiraeli,+ndichigwa chake
+17+kuyambirakuphirilaHalaki+lokwerakuSeiri+ mpakakuBaala-gadi+m’chigwachaLebanoni+m’munsi mwaphirilaHerimoni,+ndipomafumuawoonse anawagwira,+n’kuwakanthandikuwapha
18Yoswaanachitankhondondimafumuonsewokwa nthawiyaitali
19Palibemudziumeneunachitamtenderendianaa Israyeli,komaAhiviokhalam’Gibeoni; 20Yehovaanaumitsamitimayawo+kutiamenyanendi Isiraeli,+kutiawawonongekotheratu,+kutiasawakomere mtima,+komaawawononge,+mongammeneYehova analamuliraMose
+21PanthawiyoYoswaanafika+n’kuwonongaAanaki+ m’mapiri,+kuHeburoni,+kuDebiri,+kuAnabu,+ kumapirionseaYuda,+ndikumapirionseaIsiraeli +22PalibeAanaki+ameneanatsalam’dzikolaanaa Isiraeli,+komakuGaza,+kuGati,+ndikuAsidodi+ kunatsala
23MomwemoYoswaanalandadzikolonse,mongamwa zonseYehovaadauzaMose;ndipoYoswaanaliperekakwa Israyelilikhalecolowacao,mongamwamagawoao, mongamwamafukoaoNdipodzikolinapumulankhondo
MUTU12
1AwandimafumuadzikoameneanaaIsrayelianakantha, nalandadzikolawotsidyalijalaYordanokotulukiradzuwa, kuyambirakumtsinjewaArinonikufikirakuphirila Herimoni,ndichigwachonsechakum'mawa;
2SihonimfumuyaAamori,ameneanalikukhalaku Hesiboni,+ndipoanalikulamulirakuyambirakuAroweli +umeneulim’mphepetemwamtsinjewaArinoni,+ndi pakatipamtsinjewaGiliyadi,+mpakakumtsinjewa Yaboki,+umenendimalireaanaaAmoni.
3ndikuyambirakuchigwakufikirakunyanjayaKineroti kum’mawa,mpakakuNyanjayaChigwa,Nyanja Yamcherekum’mawa,njirayakuBeti-yesimoti;ndi kumwera,paAsidotiPisiga;
4NdideralaOgimfumuyaBasana,ameneanaliwa ArefaiotsalaameneanalikukhalakuAsitarotindikuEdrei. 5nakhalamfumukuphirilaHerimoni,ndikuSaleka,ndi kuBasanamonse,mpakakumalireaAgesuri,ndi Amaakati,ndihafuyaGileadi,malireaSihonimfumuya Hesiboni
6MosemtumikiwaYehovandianaaIsiraelianawakantha, ndipoMosemtumikiwaYehovaanaliperekakwaArubeni, Agadi,ndihafuyafukolaManasekutilikhalelawolawo 7AwandimafumuadzikoameneYoswandianaaIsiraeli anakanthatsidyalinalaYorodanokumadzulo,kuyambira kuBaalagadi+m’chigwachaLebanoni+mpakakuphirila Halaki+lokwerakuSeiri;limeneYoswaanapatsamafuko aIsrayelilikhalecolowacao,mongamwamagawoao; 8m’mapiri,ndim’zigwa,ndim’zidikha,ndim’zitsime,ndi m’cipululu,ndim’dzikolakumwera;ndiAhiti,ndiAamori, ndiAkanani,ndiAperizi,ndiAhivi,ndiAyebusi; 9mfumuyaYeriko,imodzi;mfumuyaAi,kufupindi Beteli,imodzi; 10mfumuyakuYerusalemu,imodzi;mfumuyaku Heburoni,imodzi; 11mfumuyakuYarimuti,imodzi;mfumuyakuLakisi, imodzi; 12mfumuyakuEgiloni,imodzi;mfumuyakuGezeri, imodzi; 13mfumuyakuDebiri,imodzi;mfumuyakuGederi, imodzi;
14mfumuyakuHorima,imodzi;mfumuyakuAradi, imodzi;
15mfumuyakuLibina,imodzi;mfumuyakuAdulamu, imodzi;
16mfumuyakuMakeda,imodzi;mfumuyakuBeteli, imodzi;
17mfumuyakuTapuwa,imodzi;mfumuyakuHeferi, imodzi;
18mfumuyakuAfeki,imodzi;mfumuyakuLasaroni, imodzi; 19mfumuyakuMadoni,imodzi;mfumuyakuHazori, imodzi; 20mfumuyakuSimironimeroni,imodzi;mfumuya Akasafu,imodzi; 21mfumuyakuTaanaki,imodzi;mfumuyakuMegido, imodzi;
22mfumuyakuKedesi,imodzi;mfumuyakuYokineamu kuKarimeli,imodzi;
23mfumuyakuDorim’mphepetemwanyanjayaDori, imodzi;mfumuyamitunduyakuGiligala,imodzi; 24mfumuyakuTiriza,imodzi;mafumuonsemakumi atatumphambummodzi
MUTU13
1NdipoYoswaanaliwokalamba,wazakazambiri;ndipo Yehovaanatikwaiye,Wakalambandiwazakazambiri, ndipopatsaladzikolambirilakukhalalako
2Dzikolotsalandiili:malireonseaAfilisti,ndiAgesuri onse;
+3KuchokerakuSihori+pafupindiIguputo+mpaka kumalireaEkroni+kumpoto,ameneankatchedwa Akanani,+mafumuasanuaAfilisiti.ndiAgaza,ndi Aasidoti,ndiAshekaloni,ndiAgiti,ndiAekroni;komanso Avites:
4Kuchokerakumwera,dzikolonselaAkanani,+ndi Meara+pafupindiAsidoni,+mpakakuAfeki,+mpaka kumalireaAamori
+5ndidzikolaAgibeli+ndiLebanonimonsekotulukira dzuwa,kuchokerakuBaala-gadi+pansipaphirila Herimoni+mpakapolowerakuHamati
+6Anthuonseokhalakuderalamapirikuyambiraku Lebanoni+mpakakuMisirefotimaimu+ndiAsidoni+ onseamenendidzawaingitsapamasopaanaaIsiraeli
7Cifukwacaceugawiredzikoililikhalecolowacamafuko asanundianai,ndihafuyafukolaManase; 8AnaaRubenindiAgadianalandiranawocholowachawo, chimeneMoseanawapatsatsidyalijalaYordano kum’mawa,mongaanawapatsaMosemtumikiwaYehova; 9KuchokerakuAroeri+umeneulim’mphepetemwa mtsinjewaArinoni,+mzindaumeneulipakatipa mtsinjewo,+ndichigwachonsechaMedeba+mpakaku Diboni; 10ndimidziyonseyaSihonimfumuyaAamori,imene inalamulirakuHesiboni,kufikirakumalireaanaaAmoni; 11ndiGileadi,ndimalireaAgesuri,ndiAmaakati,ndi phirilonselaHerimoni,ndiBasanalonse,mpakaSaleka; +12UfumuwonsewaOgi+kuBasana,+amene analamulirakuAsitaroti+ndikuEdrei,+ameneanatsala paArefai,+pakutiMoseanawakanthandi kuwathamangitsa
13KomaanaaIsrayelisanaingitsaAgesuri,kapena Amaakati; 14KomafukolaLevilokhasanawapatsecholowa;nsembe zopserezazaYehovaMulunguwaIsrayelindizocolowa cao,mongaananenanao
15NdipoMoseanapatsafukolaanaaRubenicholowa mongamwamabanjaawo.
16MalireawoanayambirakuAroeri,+umeneuli m’mphepetemwamtsinjewaArinoni,+mzindaumeneuli pakatipamtsinjewo,ndichigwachonsechaMedeba 17Hesibonindimidziyakeyonseyam’chigwa;Diboni, ndiBamoti-Baala,ndiBeti-baalameoni, 18ndiYahaza,ndiKedemoti,ndiMefaati; 19ndiKiriyataimu,ndiSibima,ndiZareti-shaharipaphiri lachigwa; 20ndiBete-peori,ndiAsidotipisiga,ndiBeti-yesimoti; 21ndimidziyonseyam’chigwa,ndiufumuwonsewa SihonimfumuyaAamori,wolamulirakuHesiboni,amene MoseanakanthapamodzindiakalongaaMidyani,Evi,ndi Rekemu,ndiZuri,ndiHuri,ndiReba,ameneanali mafumuaSihoni,okhalam’dziko
22BalamumwanawaBeori,woloserayo,anaphaanaa Israyelindilupangapakatipaiwoophedwandiiwo.
23NdipomalireaanaaRubenindiwoYordano,ndimalire akeIchichinalicholowachaanaaRubenimongamwa mabanjaawo,mizindandimidziyake.
24NdipoMoseanapatsafukolaGadi,anaaGadi,monga mwamabanjaawo,cholowa
25MalireawoanaliYazeri,+mizindayonseyaGiliyadi,+ ndihafuyadzikolaanaaAmoni,+mpakakuAroeri+ moyang’ananandiRaba
26ndikuchokerakuHesibonikufikirakuRamati-mizipe, ndikuBetonimu;ndikuyambirakuMahanaimukufikira kumalireaDebiri;
27Ndim’chigwa,Betaramu,ndiBeti-nimura,ndiSukoti, ndiZafoni,wotsalawaufumuwaSihonimfumuya Hesiboni,Yordanondimalireake,mpakakumalekezeroa nyanjayaKineretitsidyalijalaYordanokum’mawa.
28IchindicholowachaanaaGadimongamwamabanja awo,mizindandimidziyake
29NdipoMoseanapatsahafuyafukolaManasecholowa; 30MalireawoanayambirakuMahanaimu,Basanayense, ufumuwonsewaOgimfumuyaBasana,ndimidziyonse yaYairi,imeneilikuBasana,mizinda60.
31NdipohafuyaGiliyadi,+Asitaroti,+ndiEdirei,+ mizindayaufumuwaOgikuBasana,inaliyaanaaMakiri +mwanawaManase,hafuyaanaaMakiripotsata mabanjaawo
32AwandimaikoameneMoseanawagawiraakhale cholowachawom’zidikhazaMowabu,kutsidyalinala Yorodano,kuYeriko,kum’mawa
33KomafukolaLeviMosesanawapatsecholowa chilichonse;
MUTU14
1AwandimaikoameneanaaIsrayelianalandiram’dziko laKanani,ameneEleazarawansembe,ndiYoswamwana waNuni,ndiakuruamakoloamafukoaanaaIsrayeli anawagawiraakhalecholowachawo
2Cholowachawochinachitamaere,mongaYehova adalamuliramwadzanjalaMose,chamafukoasanundi anayindihafuyafuko
3PakutiMoseanapatsamafukoawirindihafucholowa tsidyalijalaYorodano,komaAlevisanawapatsecholowa pakatipawo
4PakutianaaYosefendiwomafukoaŵiri,Manasendi Efraimu;moterosanapatsaAlevigawom’dzikomo,koma
midziyokhalamo,ndimabusaaoang’ombezaondicuma cao.
5MongaYehovaanalamuliraMose,momwemoanaa Israyelianachita,nagawadziko.
6NdipoanaaYudaanadzakwaYoswakuGiligala;ndipo KalebemwanawaYefuneMkenizianatikwaiye,Udziwa iwecimeneYehovaananenandiMosemunthuwa Mulungu,zainendizaiwekuKadesi-barinea.
+7Ndinalindizaka40+pameneMosemtumikiwa YehovaananditumakuKadesi-barnea+kutindikazonde dzikondipondinambwezeramaumongandinaliri mumtimamwanga
8Komaabaleangaameneanakwerananeanasungunula mitimayaanthu,komainendinatsataYehovaMulungu wangandimtimawonse
9NdipoMoseanalumbiratsikulomwelo,kuti,Zoonadi, dzikolimenemapaziakoanapondapolidzakhalacholowa chakondichaanaakokosatha,chifukwawatsatiraYehova Mulunguwangandimtimawonse.
10Ndipotsopano,taonani,Yehovawandisungandimoyo, mongaananena,zakaizimakumianaikudzazisanu, kuyambiraYehovaananenamauawakwaMose,pamene anaaIsrayelianalikuyendayendam’cipululu;
11Ndikadaliwamphamvuleromongandinalilitsikulija Moseananditumaine:mongamphamvuyangainali nthawiyo,momwemonsomphamvuyangayankhondo, yotulukandiyolowa
12Cifukwacacetsonondipatseniphiriili,limeneYehova ananenatsikulija;pakutiunamvatsikulijakutiAanaki analikomweko,ndikutimidziinaliyaikurundiyamalinga;
13NdipoYoswaanamdalitsa,napatsaKalebemwanawa YefuneHebroniukhalecholowachake
+14ChoteroHebroniwakhalacholowachaKalebe+ mwanawaYefuneMkenizimpakalero,+chifukwa anatsatiraYehovaMulunguwaIsiraelindimtimawonse
15DzinalaHebronipoyambalinaliKiriyati-arba;amene AribaanalimunthuwamkulumwaAanaki.Ndipodziko linapumulankhondo
MUTU15
1MaereafukolaanaaYuda,mongamwamabanjaao, ndiwo;mpakakumalireaEdomu,chipululuchaZini kummwera,ndikomalekezeroakumwera
2Ndipomalireawoakum’mweraanayambirakugombela NyanjayaMchere,kuphompholoyang’anakum’mwera. 3naturukakumbaliyakumwelakuMaalehacrabimu, napitirirakuZini,nakwerakumbaliyakumwelaku Kadesi-Barinea,napitirirakuHezironi,nakwerakuAdara, nazungulirakuKarika
4KuchokerapamenepounadutsakuAzimoni+ndi kukafikakumtsinjewakuIguputo.ndimaturukiroa m’mphepetemwanyanjayoanafikirakunyanja;ndiwo ndiwomalireanuakumwera
5Malireakum’mawaanaliNyanjaYamchere+mpaka kumalekezeroaYorodanoNdimalireaokumbaliya kumpotoanacokerakuphompholanyanjakumalekezeroa Yordano;
6NdipomalirewoanakwerakuBeti-hogila,napitirira kumpotokwaBeti-araba;ndimalireanakwerakumkaku mwalawaBohanimwanawaRubeni;
7NdipomalireanakwerakumkakuDebiri,kucigwaca Akori,nakwerakumpoto,kulozakuGiligala,kulunjikaku makwereroaAdumimu,kumbaliyakumwerakwamtsinje; 8Ndipomalirewoanakweram’chigwachamwanawa Hinomu,kum’mwerakwaAyebusi;umenewondiwo Yerusalemu:ndipomalirewoanakwerapamwambapa phirilokhalapatsogolopachigwachaHinomukumadzulo, chimenechilikumapetokwachigwachaArefaikumpoto.
9Malirewoanakafikapamwambapaphirilokukafikaku kasupewamadziaNefitoa,n’kukafikakumizindaya kuphirilaEfuroni+MalirewoanakafikakuBaala,umene ndiKiriyati-yearimu
10MalirewoanazungulirakuBaala+chakumadzulo mpakakuphirilaSeiri+n’kupitirirampakakudera lamapirilaYearimu,+ndiloKesaloni,+n’kutsetserekera kuBeti-semesi+n’kupitirirampakakuTimna.
11MalirewoanapitirirampakakumbaliyaEkroni kumpoto,ndipomalirewoanakafikakuSikroni, n’kupitirirampakakuphirilaBaala,n’kupitirirampakaku Yabineelindimaturukiroamalireanalikunyanja
12MalireakumadzuloanaliNyanjaYaikulundimalire ake.LimenelindilomalireaanaaYudapozungulira potsatamabanjaawo
13NdipoanapatsaKalebemwanawaYefunegawomwa anaaYuda,mongaYehovaadauzaYoswa,mudziwa Ariba,khololaAnaki,ndiwoHebroni
14NdipoKalebeanaingitsakumenekoanaamunaatatua Anaki,Sesai,ndiAhimani,ndiTalimai,anaaAnaki.
15Kenakoanachokakumenekokupitakwaanthuokhala kuDebiri,+ndipopoyambadzinalaDebirilinaliKiriyatiseferi.
16NdipoKalebeanati,Iyeameneakanthamudziwa Kiriyati-seferi,naulanda,ndidzampatsaAkisamwana wangawamkaziakhalemkaziwake.
17NdipoOtiniyelimwanawaKenazi,mbalewakewa Kalebe,anaulanda,nampatsaAkisamwanawakewamkazi akhalemkaziwake.
18Ndipokunali,m’meneanadzakwaiye,anamkakamiza kutiapempheatatewacemunda;ndipoKalebeanatikwa iye,Ufunachiyani?
MUTU16
1NdipomaereaanaaYosefeanagwakuyambiraku YordanokuYeriko,kufikirakumadziaYerikokum’mawa, kuchipululuchokwerakuYerikokunkakuphirilaBeteli; 2naturukakuBetelikumkakuLuzi,napitiriramalirea ArikikuAtaroti;
3natsikirakumadzulokumalireaYafileti,kumalirea BetihoroniwaKunsi,ndikuGezeri;
4ChoteroanaaYosefe,ManasendiEfuraimu,anatenga cholowachawo.
5NdipomalireaanaaEfraimumongamwamabanjaao ndiwo:malireacholowachawokum’mawandiwo Atarotadara,kufikirakuBetihoroniwakumtunda; 6NdipomalirewoanaturukakumkakunyanjakuMikimeta kumpoto;Malirewoanazungulirachakum’mawampakaku Taanati-silo,n’kupitirirapokum’mawampakakuYanowa; 7natsikirakuYanowakuAtaroti,ndikuNaara,nafikaku Yeriko,naturukakuYordano.
8MalireanayambirakuTapuwakumadzulompaka kumtsinjewaKana;ndimaturukiroakeanalikunyanja
IchindicholowachafukolaanaaEfuraimupotsata mabanjaawo.
9NdipomidziyopatulidwayaanaaEfraimuinalipakati pacolowacaanaaManase,midziyonsendimidziyao.
10NdiposanaingitsaAkananiokhalakuGezeri;
MUTU17
1PanalinsomaereafukolaManase;pakutindiye woyambawaYosefe;ndiMakirimwanawoyambawa Manase,atatewaGiliyadi,popezaanalimunthu wankhondo,cifukwacaceanakhalandiGileadindiBasana 2PanalinsomaereaanaaManaseotsalamongamwa mabanjaawo;kwaanaaAbiezeri,ndianaaHeleki,ndi anaaAsiriyeli,ndianaaSekemu,ndianaaHeferi,ndiana aSemida:amenewaanalianaamunaaManasemwanawa Yosefe,mongamwamabanjaao
3KomaZelofekadi,mwanawaHeferi,mwanawaGiliyadi, mwanawaMakiri,mwanawaManase,analibeanaaamuna, komaanaaakazi,ndipomayinaaanaakeaakazindiwo Mala,ndiNowa,Hogila,Milika,ndiTiriza
4NdipoanayandikirakwawansembeEleazara,ndiYoswa mwanawaNuni,ndipamasopaakalonga,ndikuti,Yehova analamuliraMosekutipatsaifecholowapakatipaabale athu.CifukwacacemongamwalamulolaYehova anawapatsacolowapakatipaabaleaatatewao
5NdipomagawokhumianagweraManase,kuwonjezera padzikolaGileadindiBasana,okhalakutsidyalijala Yordano;
6AnaaakaziaManaseanalandiracholowapakatipaana akeaamuna,ndipodzikolaGiliyadilinakhalandiana aamunaotsalaaManase
7MalireaManaseanayambirakuAserimpakaku Mikimeta,pafupindiSekemu;ndimalireanayenda kudzanjalamanjakufikirakwaokhalakuEntapuwa 8DzikolaTapuwalinalilaManase,komaTapuwa m’malireaManaselinalilaanaaEfuraimu.
9NdipomalireanatsikirakumtsinjewaKana,kumwera kwamtsinjewo:midziiyiyaEfraimundiyopakatipamidzi yaManase;
10Kum’mwerakunalikwaEfuraimu,+kumpotokunali kwaManase,ndiponyanjayindiyomalireakenakumana kuAserikumpoto,ndiIsakarakum'mawa.
11NdipoManaseanalinaom’Isakara,ndim’Aseri, Beteseanindimidziyake,ndiIbleamundimidziyake,ndi okhalakuDorindimidziyake,ndiokhalakuEndorindi midziyake,ndiokhalam’Taanakindimidziyake,ndi okhalakuMegidondimidziyake,maikoatatu.
12KomaanaaManasesanathekuingitsaokhala m’midzimo;komaAkananianafunakukhalam’dzikomo 13Komakunali,pameneanaaIsrayelianalimbika, anasonkhetsaAkanani;komasanawaingitsakonse.
14AnaaYosefeanauzaYoswakuti:“N’chifukwachiyani mwandipatsacholowachimodzichokhandigawolimodzi, popezandineanthuambiri+chifukwaYehova wandidalitsampakapano?
15Yoswaanawayankhakuti,“Mukakhalaanthuambiri, kweranikunkhalango,+ndipomudzipatulirenokha m’dzikolaAperizi+ndilaArefai,+ngatimapiria Efuraimuakucheperani.
16NdipoanaaYosefeanati,Phirilisilitikwaniraife;ndipo Akananionseokhalam’dzikolakuchigwaalindimagareta
acitsulo,iwoakuBeti-seanindimidziyake,ndiiwoa m’chigwachaYezreeli.
17Yoswaanauzaam’nyumbayaYosefe,+Efuraimundi Manasekuti:“Inundinuanthuambiri+ndipomulindi mphamvuzambiri,+simudzakhalandigawolimodzilokha.
18Komaphirilolidzakhalalako;pakutindinkhuni,ndipo mudzaulikha,ndimaturukiroaceadzakhalaanu;
MUTU18
1NdipokhamulonselaanaaIsrayelilinasonkhanakuSilo, namangapochihemachokomanakoNdipodziko linagonjetsedwapamasopawo.
2NdipoanatsalapakatipaanaaIsrayelimafukoasanundi aŵiri,amenesanalandirebecholowachawo
3NdipoYoswaanatikwaanaaIsrayeli,Muchedwa kufikiralitikuloŵadzikolimeneYehovaMulunguwa makoloanuanakupatsani?
4Mudzipatulireamunaatatupafukolililonse,ndipo ndidzawatuma,kutianyamuke,napitepakatipadziko, nalilembemongamwacholowachawo;ndipoadzabwera kwaIne.
5Ndipoadzaligawamagawoasanundiawiri:Yuda adzakhalam’malireawokumwera,ndiam’nyumbaya Yosefeadzakhalam’malireawokumpoto.
6Cifukwacacemulembedzikomagawoasanundiawiri, nimubwerenalokunokwaine,kutindikuchitirenimaere panopamasopaYehovaMulunguwathu.
7KomaAlevialibegawopakatipanu;+Pakutiunsembe waYehovandicholowachawo,+ndipoGadindiRubeni ndihafuyafukolaManaseanalandiracholowachawo kutsidyalinalaYorodanokum’mawa,chimeneMose mtumikiwaYehovaanawapatsa
8Pamenepoamunawoananyamuka,nachoka,ndipo Yoswaanalamulaameneanapitakukalembadzikolo,+kuti: “Pitanim’dzikolo,mulilembe,+ndipomubwerekwaine, kutindikuchitirenimaere+pamasopaYehovakuSilo.
9Ndipoamunawoanapitanapitam’dzikomo,nalilemba m’bukumongamwamidzi,likhalemagawoasanundi awiri;
10NdipoYoswaanawachitiramaerekuSilopamasopa Yehova;
11NdipomaereafukolaanaaBenjaminianakwera mongamwamabanjaao;ndipomalireamaereaoanali pakatipaanaaYudandianaaYosefe
12NdipomalireawokumpotoanayambirakuYordano; nakweramalirekumbaliyaYerikokumpoto,nakwera mapirikumadzulo;ndimaturukiroaceanalikucipululuca Betaveni
13Ndipomalireanapitirirakuchokerakumenekokumka kuLuzi,kumbaliyakumwerakwaLuzi,ndikoBeteli;ndi malirewoanatsikirakuAtaroti-dara,kuphirilimenelili kumwerakwaBetihoroniWakumunsi
14Ndipomalireanaturukakumeneko,nazungulira ngondyayanyanjakum’mwera,kuchokerakuphirilimene lilimoyang’anizanandiBetihoronikum’mwera;ndi maturukiroakeanafikirakuKiriyati-baala,ndiwoKiriyatiyearimu,mudziwaanaaYuda;
15Gawolakum’mweralinayambirakumalekezeroa Kiriyati-yearimu,+ndipomalirewoanalowera chakumadzulon’kukafikakuchitsimechamadziaku Nefitoa
16Ndipomalireanatsikirakumalekezeroaphiri loyang’anizanandichigwachamwanawaHinomu, chimenechilim’chigwachaArefaikumpoto,natsikiraku chigwachaHinomu,kumbaliyaYebusikum’mwera, natsikirakuEnirogeli;
17naturukakumpoto,naturukakuEni-semesi,naturukaku Geliloti,pandunjipacitundacaAdumimu,natsikiraku mwalawaBohanimwanawaRubeni;
18napitirirakumbaliyakuArabakumpoto,natsikiraku Araba;
19MalirewoanapitirirakumbaliyakumpotokwaBetihogila,ndipomalirewoanakatherakugombelakumpoto kwaNyanjaYamchere,kumapetoakum’mwerakwa Yorodano
20NdiYordanondiyemalireakekum’mawaIchichinali cholowachaanaaBenjamini,m’malireakepozungulira ponse,mongamwamabanjaawo 21NdipomidziyapfukolaanaaBenjaminimongamwa mabanjaaondiyoYeriko,ndiBeti-hogila,ndicigwaca Kezizi; 22ndiBetaraba,ndiZemaraimu,ndiBeteli; 23ndiAvimu,ndiPara,ndiOfra, 24ndiKefara-amonai,ndiOfni,ndiGeba;midzikhumi ndiiwiri,ndimidziyao; 25Gibeoni,ndiRama,ndiBeeroti; 26ndiMizipa,ndiKefira,ndiMoza; 27ndiRekemu,ndiIripeeli,ndiTarala, 28ndiZela,ndiElefi,ndiYebusi,ndiwoYerusalemu, Gibeati,ndiKiriyati;midzikhumindiinai,ndimidziyao IchindicholowachaanaaBenjaminimongamwamabanja awo.
MUTU19
1NdipomaereachiwirianaturukakwaSimeoni,pfukola anaaSimeonimongamwamabanjaao;ndicolowacao cinalipakatipacolowacaanaaYuda.
2Ndipom’cholowachawoanalindiBeereseba,kapena Seba,ndiMolada;
3ndiHazarasuali,ndiBala,ndiAzemu, 4ndiElitoladi,ndiBetuli,ndiHorima; 5ndiZikilagi,ndiBetimarakaboti,ndiHazarasusa; 6ndiBetelebaoti,ndiSaruheni;midzikhumindiitatu,ndi midziyao;
7Aini,Remoni,ndiEteri,ndiAsani;midziinaindimidzi yao;
8Ndimidziyonseyozunguliramidziimeneyimpakaku Baalati-beeri,+mzindawaRama+wakum’mwera.Ichi ndicholowachafukolaanaaSimeonimongamwa mabanjaawo
9CholowachaanaaSimiyonichinalipagawolaanaa Yuda,pakutigawolaanaaYudalinawakulira; 10Maereachitatu+anagweraanaaZebuloni+monga mwamabanjaawo,ndipomalireacholowachawoanafika kuSaridi
11Ndipomalireaoanakwerakumkakunyanja,ndiku Marala,nakafikakuDabaseti,nakafikakumtsinjewaku Yokineamu;
12KufumakuSaridiwakafumakuSaridikukapindakaku kusokukapindakakukulyokukabangaukuyakumupaka waKisloti-tabori,kabiliatutukilekuDaberatinokuyaku Yafia
13Kucokerakumenekoanapitirirakum’mawakumkaku Gitaheferi,kuItazanini,naturukakuRemoni-metowariku Nea;
14Malirewoanazunguliraderalakumpoton’kukafikaku Hanatoni,n’kukatherakuchigwachaIfitaeli.
15ndiKatati,ndiNahalala,ndiSimironi,ndiIdala,ndi Betelehemu;midzikhumindiiwirindimidziyake
16IchindicholowachaanaaZebulonimongamwa mabanjaao,midziiyindimiragayao
17MaereachinayianagweraIsakara,+anaaIsakara mongamwamabanjaawo
18NdimalireaoanafikirakuYezireeli,ndiKesuloti,ndi Sunemu;
19ndiHafaraimu,ndiSioni,ndiAnaharati, 20ndiRabiti,ndiKisioni,ndiAbezi; 21ndiRemeti,ndiEnganimu,ndiEnihada,ndiBetepaze; 22MalirewoanafikakuTabori,kuSahazuma,ndikuBetisemesi;ndimalekezeroamalireaoanalikuYordano; midzikhumindiisanundiumodzindimiragayao. 23IchindicholowachafukolaanaaIsakaramongamwa mabanjaawo,mizindandimidziyake
24MaereachisanuanatulukirafukolaanaaAserimonga mwamabanjaawo
25NdimalireaondiwoHelekati,ndiHali,ndiBeteni,ndi Akasafu;
26ndiAlameleki,ndiAmadi,ndiMisela;nafikiraku Karimelikumadzulo,ndikuSihori-libinati;
27nakhoterakotulukiradzuwakuBeti-dagoni,nafikiraku Zebuloni,ndikuchigwachaIfetahelekumpotokwa Betemeki,ndiNeyeli,naturukakuKabulikudzanja lamanzere;
28ndiHebroni,ndiRehobu,ndiHamoni,ndiKana, kufikirakuZidoniwaukulu;
29KenakomalirewoanalowerakuRama,+mpakaku mzindawaTuro+wokhalandimpandawolimbakwambiri ndimalirewoanatembenukirakuHosa;naturukakunyanja, kucokeram’mphepetemwanyanjakumkakuAkizibu; 30Umanso,ndiAfeki,ndiRehobu;midzimakumiawiri mphambuiwirindimiragayao
31IchindicholowachafukolaanaaAserimongamwa mabanjaao,midziiyindimiragayao
32MaereachisanundichimodzianagweraanaaNafitali, ndiwoanaaNafitalimongamwamabanjaao.
33NdimalireaoanayambirakuHelefi,kuAlon,kufikira Zaananimu,ndiAdami,Nekebu,ndiYabineeli,kufikira Lakumu;ndimatheroakeanalipaYordano;
34MalirewoanakhoterakumadzulokuAzinoti-tabori,+ n’kuchokerakumenekon’kukafikakuHukoki,+ n’kukafikakuZebuloni+kum’mwera,n’kukafikakuAseri +kumadzulo,ndikuYudapaYorodanokotulukiradzuwa 35NdimidziyamalingandiyoZidimu,Zeri,ndiHamati, Rakati,ndiKinereti; 36ndiAdamu,ndiRama,ndiHazori, 37ndiKedesi,ndiEdirei,ndiEnihazori; 38ndiIroni,ndiMigidaleli,Horemu,ndiBetanati,ndi Beti-semesi;midzikhumindiisanundiinai,ndimidziyao 39IchindicholowachafukolaanaaNafitalimongamwa mabanjaawo,midzindimidziyake
40MaereachisanundichiwirianagwerafukolaanaaDani mongamwamabanjaawo.
41NdipomalireacolowacaondiwoZora,ndiEsitaoli,ndi Isimesi;
42ndiSaalabini,ndiAjaloni,ndiYetila; 43ndiEloni,ndiThimnata,ndiEkroni; 44ndiEliteke,ndiGibetoni,ndiBaalati; 45ndiYehudi,ndiBeneberaka,ndiGatirimoni; 46ndiMeyarikoni,ndiRakoni,ndimalireakuYafo.
47NdipomalireaanaaDanianawachepera;chifukwa chakeanaaDanianakwerakukamenyanandiLesemu, naulanda,naukanthandilupangalakuthwa,naulanda, nakhalam’menemo;
48IchindicholowachafukolaanaaDanimongamwa mabanjaao,midziiyindimiragayao
49Atathakugawadzikolomongacholowachawo,+anaa IsiraelianapatsaYoswamwanawaNunicholowapakati pawo
50MogwirizanandimawuaYehovaanam’patsamzinda umeneanaupempha,+mzindawaTimnati-sera+m’dera lamapirilaEfuraimu
51IzindizolowazimeneEleazarawansembe,ndiYoswa mwanawaNuni,ndiatsogoleriamakoloamafukoaanaa Israyeli,anazigawirapochitamaerekuSilopamasopa Yehova,pakhomolachihemachokomanakoChoncho anamalizakugawadziko.
MUTU20
1YehovaananenansondiYoswa,nati, 2NenandianaaIsrayeli,ndikuti,Mudzisankhiremidzi yopulumukirako,imenendinanenandiinumwadzanjala Mose;
3kutiwakuphamunthumosadziŵaathawireko,ndipo akhalepothawirapopawolipsiramwazi.
4Ndipoakathawirakuumodziwamidziimeneyo, akaimirirapolowerapachipatachamzindawo,nakanena mlanduwakem’makutuaakuluamudziwo,amtengere kumzindakwaiwo,ndikumpatsamalo,kutiakhalepakati pao
5Ndipowolipsirawamwaziakamlondola,asapereke wakupham’dzanjalake;popezaanakanthamnansiwake mosadziwa,osamudakale
6Ndipoazikhalam’mudziumenewo,kufikiraataimirira pamasopakhamukutiaweruze,kufikiraatafamkuluwa ansembewakukhalam’masikuamenewo;pamenepo wakuphawakuphayoazibweransokumzindawake,ndi kunyumbakwake,kumzindaumeneanathawirako
7NdipoanaikaKedesim’Galileyam’phirilaNafitali,ndi Sekemum’deralamapirilaEfraimu,ndiKiriyati-araba, ndiwoHebroni,m’phirilaYuda
8NditsidyalinalaYorodanopaYerikochakum’maŵa, anapatsaBezerim’chipululum’chigwapafukolaRubeni, ndiRamotim’GiliyadipafukolaGadi,ndiGolani m’BasanawafukolaManase
9IyindiyomidziyoikiraanaonseaIsrayeli,ndimlendo wokhalapakatipawo,kutialiyensewakuphamunthudala athawireko,kutiasafendidzanjalawolipsiramwazi, kufikiraataimapamasopamsonkhano
MUTU21
1PamenepoakuluamakoloaAlevianayandikirakwa wansembeEleazara,ndiYoswamwanawaNuni,ndikwa akuluamakoloamafukoaanaaIsraele;
2NdipoananenanawokuSilom’dzikolaKanani,kuti, YehovaanalamuliramwadzanjalaMose,kutipatsamidzi yokhalamo,ndimabusaang’ombezathu
3NdipoanaaIsrayelianapatsaAlevimidziiyindimabusa ao,pacolowacao,mongamwalamulolaYehova.
4NdipomaereanagweramabanjaaAkohati;ndipoanaa Aroniwansembe,ndiwoaAlevi,analandiramwamaerepa fukolaYuda,ndipafukolaSimeoni,ndipafukola Benjamini,midzikhumindiitatu
5NdipoanaaKohatiotsalaanalandiramwamaerepa mabanjaafukolaEfraimu,ndipafukolaDani,ndipahafu lafukolaManase,midzikhumi
6NdipoanaaGerisonianalandiramwamaerepamabanja afukolaIsakara,ndipafukolaAseri,ndipafukola Nafitali,ndipahafulafukolaManasekuBasana,midzi khumindiitatu.
7AnaaMerarimongamwamabanjaaoanalandiramidzi khumindiiwiri,motapapafukolaRubeni,ndipafukola Gadi,ndipafukolaZebuloni.
8NdipoanaaIsrayelianaperekamwamaerekwaAlevi midziiyindimabusaake,mongaYehovaadalamuliramwa dzanjalaMose.
9NdipoanapatsapapfukolaanaaYuda,ndipapfukola anaaSimiyoni,midziiyiyochulidwamainaao;
10AnaaAroni,amabanjaaAkohati,obadwaaanaaLevi, analinazo;pakutimaereoyambandiwoanawagwera
11NdipoanawapatsamudziwaAriba,atatewaAnaki, ndiwoHebroni,m’deralamapirilaYuda,ndimabusaake ozungulirapake
12Komamindayamzindawondimidziyakeanapatsa KalebemwanawaYefunezikhalezake.
13MomwemoanapatsaanaaAroniwansembeHebroni ndimabusaake,ukhalemudziwopulumukirakowakupha munthu;ndiLibinandimabusaake,
14ndiYatirindimabusaace,ndiEsitemowandimabusa ace;
15ndiHolonindimabusaace,ndiDebirindimabusaace; 16ndiAinindimabusaake,Yutandimabusaake,Betisemesindimabusaake;midziisanundiinayimwamafuko awiriwo.
17NdipomotapirakufukolaBenjamini,Gibeonindi mabusaace,Gebandimabusaace;
18Anatotindimabusaake,ndiAlimonindimabusaake; midziinayi
19MizindayonseyaanaaAroni,ansembe,ndiyomidzi khumindiitatu,ndimabusaake.
20NdipomabanjaaanaaKohati,Aleviotsalaaanaa Kohati,analandiramidziyamaereaopafukolaEfraimu. 21AnawapatsaSekemu+ndimabusaake+m’dera lamapirilaEfuraimu,+kutiukhalemzinda wopulumukirakowakuphamunthundiGezerindimabusa ake;
22ndiKibizaimundimabusaake,Betihoronindimabusa ake;midziinayi
23NdipomotapirakufukolaDani,Elitekendimabusaace, Gibetonindimabusaace; 24Aiyalonindimabusaake,Gatirimonindimabusaake; midziinayi
25NdipomotapirapahafuyafukolaManase,Tanakindi mabusaake,ndiGatirimonindimabusaake;midziiwiri.
26MizindayonseyamabanjaaanaaKohatiotsalawoinali khumindimabusaake
27AnaaGerisoni,amabanjaaAlevi,anawapatsa,pahafu yafukolaManase,GolanikuBasanandimabusaake, mudziwopulumukirakowakuphamunthu;ndiBeesitera ndimabusaake;midziiwiri.
28NdipomotapirakufukolaIsakara,Kisonindimabusa ake,Dabarendimabusaake; 29Yarimutindimabusaake,Enganimundimabusaake; midziinayi.
30NdipomotapirafukolaAseri,Misalindimabusaake, Abidonindimabusaake;
31Helikatindimabusaake,ndiRehobundimabusaake; midziinayi
32Ndipokuchokeram’fukolaNafitali,Kedesi+ m’Galileyandimabusaake,+mzindawopulumukirako wakuphamunthu;ndiHamotidorindimabusaace,ndi Karitanindimabusaace;midziitatu.
33MizindayonseyaAgerisonimongamwamabanjaao ndiyomidzikhumindiitatu,ndimabusaao
34NdikwamabanjaaanaaMerari,otsalaaAlevi,pafuko laZebuloni,Yokineamundimabusaake,ndiKartandi mabusaake;
35Dimnandimabusaake,Nahalalindimabusaake;midzi inayi
36NdipomotapirakufukolaRubeni,Bezerindimabusa ake,ndiYahazandimabusaake;
37Kedemotindimabusaake,Mefaatindimabusaake; midziinayi
38NdipomotapirafukolaGadi,Ramotim’Giliyadindi mabusaace,ndiwomudziwopulumukirakowakupha munthu;ndiMahanaimundimabusaake,
39Hesibonindimabusaake,Yazerindimabusaake;midzi inaiyonse
40MomwemomidziyonseyaanaaMerarimongamwa mabanjaao,otsalaamabanjaaAlevi,inakhalamidzi khumindiiwirim’maereao
41MizindayonseyaAlevipakatipacholowachaanaa Israyelindiyomidzimakumianaikudzaisanundiitatu,ndi mabusaake
42Mizindaiyiinaliyonsendimabusaakeoizungulira;
43NdipoYehovaanapatsaIsrayelidzikolonselimene analumbirirakuwapatsamakoloao;nalilandira,nakhala m’menemo
44Yehovaanawapatsampumulopozunguliraponse, mongamwazonseanalumbiriramakoloawo;Yehova anaperekaadaniawoonsem’manjamwawo
45Sipanasowekanthukalikonsekazinthuzabwinozonse zimeneYehovaanalankhulakwanyumbayaIsiraeli;zonse zidachitika.
MUTU22
1NdipoYoswaanaitanaArubeni,ndiAgadi,ndihafuya fukolaManase,
2natikwaiwo,MunasungazonseMosemtumikiwa Yehovaanakulamulirani,ndikumveramauangam’zonse ndinakulamuliraniinu;
3Simunasiyeabaleanumasikuambiriawampakalero, komamwasungaudikirowalamulolaYehovaMulungu wanu
4NdipotsopanoYehovaMulunguwanuwapumulitsa abaleanu,mongaanawalonjezera;
5Komamusamalirekuchitalamulondichilamulochimene MosemtumikiwaYehovaanakulamulirani,kukonda YehovaMulunguwanu,ndikuyendam’njirazakezonse, ndikusungamalamuloake,ndikum’mamatira,ndi kum’tumikirandimtimawanuwonse,ndimoyowanu wonse
6ChoteroYoswaanawadalitsa+n’kuwalolakutiazipita,+ ndipoanapitakumahemaawo.
7NdipohafuyafukolaManaseMoseanapatsacholowa chakekuBasana;NdipopameneYoswaanawalolaamuke kumahemaao,nawadalitsa;
8Ndipoananenanao,nati,Bwereranikumahemaanundi chumachambiri,nding’ombezambirimbiri,ndisiliva,ndi golidi,ndimkuwa,ndichitsulo,ndizovalazambirimbiri;
9NdipoanaaRubeni,ndianaaGadi,ndihafuyafukola Manaseanabwerera,nachokakwaanaaIsrayelikuSilo, m’dzikolaKanani,kunkakudzikolaGileadi,kudzikola cholowachawo,limeneadalandira,mongamwamawua YehovamwadzanjalaMose.
10NdipoatafikakumalireaYordano,okhalam’dzikola Kanani,anaaRubeni,ndianaaGadi,ndihafuyafukola Manase,anamangakumenekoguwalansembe m’mphepetemwaYordano,guwalansembelalikuru 11NdipoanaaIsrayelianamvakuti,Taonani,anaa Rubeni,ndianaaGadi,ndihafuyafukolaManase amangaguwalansembepopenyanandidzikolaKanani, m’malireaYordano,poloweraanaaIsrayeli
12AnaaIsiraeliatamvazimenezi,khamulonselaanaa IsiraelilinasonkhanakuSilokutiakamenyanenawo
13NdipoanaaIsrayelianatumizakwaanaaRubeni,ndi kwaanaaGadi,ndihafuyafukolaManase,kudzikola Gileadi,PinehasimwanawaEleazarawansembe; 14ndipamodzinayeakalongakhumi,kalongam’mafuko onseaIsrayeliwanyumbayamfumu;+ndipoaliyense analimtsogoleriwanyumbayamakoloawomwa masauzandeaIsiraeli
15NdipoanafikakwaanaaRubeni,ndikwaanaaGadi, ndihafuyafukolaManase,m’dzikolaGileadi,nanena nao,ndikuti,
16KhamulonselaYehovalikunenakuti,‘Cholakwa chotanichimenemwalakwiraMulunguwaIsiraelin’kusiya kutsatiraYehovalero,+podzimangiraguwalansembe+ kutimupandukireYehovalerolino?
17KodicholakwachaPeorindichaching’onokwaife,+ chimenesitinayeretsedwe+nachompakalero,+ngakhale kutipanalimlirimumpingowaYehova?
18KomakodimupatukalerokusatsataYehova?ndipo kudzakhala,popezamukupandukiraYehovalero,mawa adzakwiyirakhamulonselaIsrayeli
19Komadzikolacholowachanulikakhalalodetsedwa, muolokem’dzikolacholowachanuchaYehova,m’mene mukhalachihemachaYehova,nimulandirecholowapakati pathu;
20KodiAkanimwanawaZerasanalakwepachinthu choperekedwachoperekedwacho,ndipomkwiyounagwera khamulonselaIsiraeli?ndipomunthuyosanaonongeka yekham’mphulupuluyace.
21PamenepoanaaRubeni,ndianaaGadi,ndihafuya fukolaManaseanayankha,natikwaatsogoleriazikwiza Israyeli,
22YehovaMulunguwamilungu,YehovaMulunguwa milungu,iyeadziŵa,ndipoIsrayeliadzadziŵa;ngatindi
Yoswa
kupandukira,kapenakulakwiraYehova,(musatipulumutse lero,)
+23kutitadzimangiraguwalansembe+kutitisiye kutsatiraYehova,+kapenakuperekaponsembeyopsereza, +kapenansembeyambewu,+kapenakutitizipherapo nsembezachiyanjano,+Yehovaafunefune
24Ngatisitinachitezimenezichifukwachoopazimenezi,+ kuti,‘M’tsogoloanaanuadzauzaanaathukuti,‘Mulindi chiyanindiYehovaMulunguwaIsiraeli?
25YehovawaikaYordanokukhalamalirepakatipaifendi inu,anaaRubenindianaaGadi;mulibegawomwa Yehova;moteroanaanuadzalekaanaathukuopaYehova 26Cifukwacacetinati,Tiyenitikonzetukudzimangira guwalansembe,silansembeyopsereza,kapenalansembe; 27Komakutiukhalembonipakatipaifendiinu,ndi mibadwoyathuyapambuyopathu,kutitichiteutumikiwa Yehovapamasopakendinsembezathuzopsereza,ndi nsembezathu,ndinsembezathuzamtendere;kutianaanu anganenekwaanaathum’tsogolomo,Mulibegawomwa Yehova
28Chifukwachaketidati,padzakhala,pameneadzatiuza ifekapenamibadwoyathum’tsogolo,tidzanenanso, TaonanichitsanzochaguwalansembelaYehova,limene makoloathuanapanga,silansembezopsereza,kapenala nsembe;Koma(Qur'an)ndimboniPakatipathundiinu.
29MulungualekenikutitipandukireYehova,ndi kutembenukalerokusiyakutsatiraYehova,kumangaguwa lansembezopsereza,lansembezaufa,kapenalansembe, pambalipaguwalansembelaYehovaMulunguwathu limenelilipatsogolopachihemachake
30NdipoPinehasiwansembe,ndiakalongaakhamulo,ndi atsogoleriazikwizaIsrayeliameneanalinaye,anamva mauameneanaaRubeni,ndianaaGadi,ndianaaManase ananena,chinawakomera.
31NdipoPinehasimwanawaEleazarawansembeanati kwaanaaRubeni,ndianaaGadi,ndianaaManase,Lero tazindikirakutiYehovaalipakatipathu,popeza simunalakwiraYehova;tsopanomwalanditsaanaaIsrayeli m’dzanjalaYehova
32NdipoPinehasimwanawawansembeEleazara,ndi akalonga,anabwererakuchokerakwaanaaRubeni,ndi kwaanaaGadi,m’dzikolaGileadi,kunkakudzikola Kanani,kwaanaaIsrayeli,nawabwezeramau.
33NdipochinthuchochinakomeraanaaIsrayeli;ndipoana aIsrayelianalemekezaMulungu,osafunakuwakwerera kunkhondo,kukaonongadzikom’meneanaaRubenindi Gadianakhalamo
34NdipoanaaRubenindianaaGadianatchaguwaloEdi, pakutindilombonipakatipathukutiYehovandiye Mulungu
MUTU23
1Ndipopanaliatapitamasikuambiri,Yehovaatapumitsa Israyelikwaadaniaoonseowazungulira,Yoswa anakalambanakalamba
2NdipoYoswaanaitanaAisrayelionse,ndiakuluao,ndi akuruao,ndioweruzaao,ndiakapitaoao,nanenanao, Ndakalamba,ndizakazambiri;
3NdipoinumunapenyazonseYehovaMulunguwanu anachitiramitunduiyiyonsechifukwachainu;pakuti
YehovaMulunguwanundiyeameneanakumenyerani nkhondo.
4Taonani,ndakugawiranindimaereamitunduawa otsalawo,akhalecholowachamafukoanu,kuyambirapa Yordano,ndiamitunduonseamenendinawapasula, kufikirakunyanjayaikulukumadzulo
5NdipoYehovaMulunguwanuadzawaingitsapamaso panu,ndikuwaingitsakuwachotsapamasopanu;ndipo mudzalandiradzikolao,mongaYehovaMulunguwanu anakulonjezani
6Cifukwacacekhalaniolimbikamtimandithu,kusunga ndikucitazonsezolembedwam’bukulacilamulocaMose, kutimungapatukirekokulamanjakapenakulamanzere; 7kutimungalowemwaamitunduawaotsalamwainu; musatchuledzinalamilunguyao,kapenakulumbiritsapa iyo,kapenakuitumikira,kapenakuigwadira;
8KomagwiritsitsaniYehovaMulunguwanu,monga mwachitampakalero
9PakutiYehovaanaingitsapamasopanumitunduyaikuru ndiyamphamvu;komainu,palibemunthuanaimapamaso panukufikiralerolino
+10Munthummodziwainuadzathamangitsaanthu1,000, +pakutiYehovaMulunguwanundiyeamene amakumenyeraninkhondo+mongammeneanalonjezera
11Cifukwacacemudzicenjere,kutimukondeYehova Mulunguwanu
12Kapenamukabwereram’mbuyo,ndikumamatiraotsala aamitunduawa,ndiwootsalamwainu,ndikukwatirana nawo,ndikulowakwaiwo,ndiiwowokwainu;
13DziwanindithukutiYehovaMulunguwanu sadzaingitsansoamitunduawapamasopanu;koma adzakhalakwainumisamphandimisampha,ndizikwapu m’nthitimwanu,ndimingam’masomwanu,kufikira mutatayikam’dzikolokomaililimeneYehovaMulungu wanuwakupatsani
14Ndipotaonani,lerondiyendanjirayadzikolonse lapansi;zonsezidachitikirainu,ndipopalibechinthu chimodzichalephera
15Cifukwacacekudzakhalakuti,mongazakugwerani zabwinozonse,zimeneYehovaMulunguwanu anakulonjezani;momwemoYehovaadzakutengeranizoipa zonse,kufikiraatakuononganikukuchotsanim’dziko lokomailiYehovaMulunguwanuwakupatsani.
16MukalakwirapanganolaYehovaMulunguwanu, limeneanakulamulirani,ndikupitakukatumikiramilungu ina,ndikuigwadira;pamenepomkwiyowaYehova udzakuyakirani,ndipomudzaonongekamsangam’dziko labwinolimeneanakupatsani.
MUTU24
1NdipoYoswaanasonkhanitsamafukoonseaIsrayeliku Sekemu,naitanaakuluaIsrayeli,ndiakuruao,ndi oweruzaao,ndiakapitaoao;ndipoanadzionetserapamaso paMulungu
2Yoswaanauzaanthuonsewokuti:“YehovaMulunguwa Isiraeliwanenakuti,‘Kalemakoloanuanalikukhalatsidya linalaMtsinje,ndiyeTera,bamboakeaAbulahamundi Nahori,+ndipoankatumikiramilunguina
3NdipondinatengaatatewanuAbrahamutsidyalijala chigumula,ndikumtsogoleraiyem’dzikolonselaKanani, ndikuchulukitsambewuzake,nampatsaiyeIsake
4NdipondinapatsakwaIsakeYakobondiEsau:ndipo ndinapatsaEsauphirilaSeirilikhalelake;komaYakobo ndianaakeanatsikirakuAigupto
5NdinatumizansoMosendiAroni,ndipondinakantha Aigupto,mongandinachitirapakatipao;ndipopambuyo pakendinakuturutsani
6NdipondinaturutsamakoloanukuAigupto,ndipo munafikakunyanja;ndipoAaiguptoanalondolamakolo anundimagaretandiapakavalokufikirakuNyanjaYofiira 7NdipopameneanapfuulirakwaYehova,iyeanaika mdimapakatipainundiAaigupto,natengeranyanjapa iwo,nawaphimba;ndipomasoanuanawonachimene ndinachitam’Aigupto:ndipomunakhalam’chipululu masikuambiri
8Ndipondinakulowetsanim’dzikolaAamori,okhala tsidyalijalaYordano;ndipondinawaperekam'dzanjalanu, kutimutengedzikolao;ndipondinawaonongapamaso panu
9PamenepoBalakimwanawaZipori,mfumuyaMoabu, anaukanamenyanandiIsrayeli,natumizanaitanaBalamu mwanawaBeorikutiakutemberereni; 10KomasindinafunakumveraBalamu;cifukwacace anakudalitsanibe,ndipondinakulanditsanim'dzanjalace 11NdipomunaolokaYorodanondikukafikakuYeriko, ndipoamunaakuYerikoanakuthirankhondoAamori,ndi Aperizi,ndiAkanani,ndiAhiti,ndiAgirigasi,Ahivi,ndi Ayebusi;ndipondinawaperekam’dzanjalanu
12Ndipondinatumizamavupatsogolopanu,amene anawaingitsapamasopanu,ndiwomafumuawiriaAamori; komasindilupangalako,kapenandiutawako
13Ndipondinakupatsanidzikolimenesimunagwirirapo ntchito,ndimidziimenesimunaimanga,ndipomukhalamo; Mumadyazamindayamphesandiazitonazimene simunaoka.
14TsopanoopaniYehova,+mum’tumikiremoonamtima +ndim’choonadi,+ndipochotsanimilunguimenemakolo anuankaitumikirakutsidyalinalaChigumula+ndiku IguputondipotumikiraniYehova
15NdipongatikutumikiraYehovakukuipirani,sankhani leroamenemudzamtumikira;kapenamilunguimene makoloanuanaitumikiratsidyalijalamtsinjewo,kapena milunguyaAamori,amenemukhalam’dzikolao;koma inendiam’nyumbayanga,tidzatumikiraYehova.
16Ndipoanthuanayankha,nati,Kulekenikwathukumsiya Yehova,ndikutumikiramilunguyina; 17PakutiYehovaMulunguwathu,ndiyeamene anatitulutsaifendimakoloathum’dzikolaAigupto, m’nyumbayaukapolo,nachitazizindikirozazikuluzo pamasopathu,ndikutisungam’njirayonsem’mene tinayendamo,ndimwaanthuonseamenetinadutsamo; 18NdipoYehovaanaingitsapamasopathumitunduyonse yaanthu,Aamoriokhalam’dziko;pakutindiyeMulungu wathu
19NdipoYoswaanatikwaanthu,Simungathekutumikira Yehova,popezaiyendiyeMulunguwoyera;ndiye Mulunguwansanje;sadzakhululukirazolakwazanukapena zolakwazanu.
20MukasiyaYehova,ndikutumikiramilunguyachilendo, iyeadzatembenuka,nadzakuchitiranichoipa,ndikuthainu, atakuchitiranizabwino.
21NdipoanthuanatikwaYoswa,Iai;komaife tidzatumikiraYehova
22Yoswaanauzaanthuwokuti:“Inundinumbonipainu nokhakutimwasankhaYehovakutimumutumikire.Ndipo adati,Ndifemboni
+23Choterochotsanimilunguyachilendo+imeneili pakatipanu,+ndipomulozetsemitimayanukwaYehova MulunguwaIsiraeli
24NdipoanthuanatikwaYoswa,YehovaMulunguwathu tidzamtumikira,ndipotidzamveramawuake.
25ChoteroYoswaanachitapanganondianthuwotsiku lomwelo,nawaikiralembandilembam’Sekemu
26NdipoYoswaanalembamawuawam’bukula chilamulochaMulungu,natengamwalawaukulu, nauimikapamenepopansipamtengowaukulu,umene unalipafupindimaloopatulikaaYehova
27NdipoYoswaanatikwaanthuonse,Taonani,mwala uwuukhalembonikwaife;pakutilamvamauonsea Yehovaameneananenakwaife;cifukwacacelikhale mbonikwainu,mungakaneMulunguwanu
28PamenepoYoswaanalolaanthuamuke,yenseku cholowachake
29Ndipokunalizitapitaizi,YoswamwanawaNuni, mtumikiwaYehova,anamwalira,alindizakazanalimodzi kudzakhumi
30Ndipoanamuikam’malireacholowachakem’Timinatisera,m’deralamapirilaEfuraimu,kumpotokwaphirila Gaasi
+31AisiraelianatumikiraYehova+masikuonseaYoswa, +ndimasikuonseaakuluameneanakhalabendimoyo Yoswa,+ameneankadziwantchitozonsezimeneYehova anachitiraAisiraeli
32NdipomafupaaYosefe,ameneanaaIsrayelianakwera kucokerakuAigupto,anawaikam’Sekemu,m’gawola nthakalimeneYakoboanagulakwaanaaHamoriatatewa Sekemundindalamazasilivazanalimodzi;
33NdipoanafaEleazaramwanawaAroni;+Kenako anamuikam’mandapaphirilaPinehasi+mwanawake, limeneanam’patsam’deralamapirilaEfuraimu.