Chichewa - The First Epistle of John

Page 1


EpistolaWoyamba waYohane

MUTU1

1Chimenechidalikuyambirapachiyambi,chimene tidachimva,chimenetidachiwonandimasoathu,chimene tidachipenyerera,ndipomanjaathuadachigwira,cha Mawuamoyo;

2(Pakutimoyounaonekera,ndipotinauona,ndipotichita umboni,ndipotikulalikiranimoyowosathaumeneunali ndiAtate,ndipounaonekerakwaife;)

3Chimenetinachiwonandikumva,tikulalikiranikwainu, kutiinunsomukhalenachochiyanjanondiife:ndipo ndithudichiyanjanochathuchirindiAtate,ndiMwana wakeYesuKhristu

4Ndipoizitikulemberani,kutichimwemwechanu chisefukire.

5NdipouwundiuthengatidaumvakwaIye,ndipo tiulalikirakwainu,kutiMulungundiyekuunika,ndipo mwaIyemulibemdimakonse

6TikanenakutitiyanjanandiIye,ndipotikuyenda mumdima,tinama,ndipositicitacoonadi;

7Komangatitiyendam’kuunika,mongaIyealim’kuunika, tiyanjanawinandimnzake,ndipomwaziwaYesuMwana wakeutisambitsakutichotserauchimowonse.

8Tikanenakutitilibeuchimo,tidzinyengatokha,ndipo mwaifemulibechoonadi

9Ngatitivomerezamachimoathu,aliwokhulupirikandi wolungamaIye,kutiatikhululukiremachimoathu,ndi kutisambitsakutichotserachosalungamachilichonse

10Tikanenakutisitinacimwa,tiyesaIyewonama,ndipo mwaifemulibemauake

MUTU2

1Tianatanga,izindakulemberani,kutimusachimwe Ndipoakachimwawina,nkhoswetirinayekwaAtate, ndiyeYesuKristuwolungama;

2Iyendiyechiwombolochamachimoathu,osatiathuokha, komansoadzikolonselapansi.

3UmotizindikirakutitamzindikiraIye,ngatitisunga malamuloake

4Iyewakunenakuti,Ndikumudziwa,komasasunga malamuloake,ndiwabodza,ndipomwaiyemulibe choonadi

5Komaiyeameneasungamawuake,mwaiyendithu chikondichaMulunguchikhalachangwiro;

6Iyeameneanenakutiakhalamwaiyeayeneranso kuyendamongammeneiyeanayendera.

7Abale,sindikulemberanilamulolatsopano,komalamulo lakalelimenemunalinalokuyambirapachiyambiLamulo lakalendilomauamenemudawamvakuyambira pachiyambi

8Ndiponso,ndikulemberanilamulolatsopano,limenelili loonamwaiyendimwainu;

9Iyewakunenakutialim’kuunika,nadanandimbalewake, alimumdimakufikiratsopanolino.

10Iyeameneakondambalewakeakhalam’kuunika,ndipo mwaiyemulibechokhumudwitsa

11Komaiyeameneadanandimbalewakealimumdima, nayendamumdima,ndiposadziwakumeneamukako, chifukwamdimawamchititsakhungumasoake

12Ndikulemberani,tiana,chifukwamachimoanu akhululukidwachifukwachadzinalake

13Ndikulemberani,atate,chifukwamwadziwaIyeamene alikuyambirapachiyambi.Ndikulemberani,anyamata, chifukwamunagonjetsawoipayoNdikulemberani,tiana, chifukwamwadziwaAtate

14Ndakulemberani,atate,chifukwamwadziwaIyeamene alikuyambirapachiyambiNdalembakwainu,anyamata, chifukwamuliamphamvu,ndimawuaMulunguakhala mwainu,ndipomunagonjetsawoipayo.

15Musakondedzikolapansi,kapenazam’dzikolapansi Ngatiwinaakondadzikolapansi,chikondichaAtatesichili mwaiye.

16Pakutizonsezam’dzikolapansi,chilakolakochathupi, chilakolakochamaso,matamandidweamoyo,sizichokera kwaAtate,komakudzikolapansi.

17Ndipodzikolapansilipita,ndichilakolakochake; 18Tiana,inondinthawiyotsiriza:ndipomongamudamva kutiwokanaKhristuadzafika,ngakhaletsopanoalipo okanaKhristuambiri;m’menemotidziwakutindinthawi yotsiriza

19Adatulukamwaife,komasanaliaife;pakuti akadakhalaaife,akadakhalabendiife;

20KomainumudadzozedwandiWoyerayo,ndipo mudziwazinthuzonse

21Sindinakulemberanichifukwasimudziwachowonadi, komachifukwamukuchidziwa,ndikutipalibebodza lomwelimachokeram'chowonadi

22WabodzandanikomaiyeameneakanakutiYesusi Khristu?IyealiwokanaKhristu,ameneakanaAtatendi Mwana.

23YensewakukanaMwana,yemweyoalibeAtate;(koma) iyeameneabvomerezaMwanaalindiAtatenso.

24Chifukwachakelolanikutichimenemudachimva kuyambirapachiyambichikhalemwainuNgatichimene mudachimvakuyambirapachiyambichikhalamwainu, inunsomudzakhalamwaMwana,ndimwaAtate 25NdipoilindilonjezolimeneIyeanatilonjeza,ndilo moyowosatha.

26Zinthuizindakulemberanizaiwoakusokeretsainu

27KomakudzozakumenemudalandirakwaIyekukhala mwainu,ndiposimusowakutiwinaakuphunzitseni;inu, mudzakhalamwaIye

28Ndipotsopano,tiana,khalanimwaIye;kuti pakuwonekeraIye,tikhalenakokulimbikamtima,ndi kusachitamanyazipamasopakepakudzakwake

29Ngatimudziwakutialiwolungama,dziwanikutiyense wakuchitachilungamoabadwakuchokerakwaiye.

MUTU3

1Taonani,chikondichoAtatewatipatsa,kutititchedweana aMulungu;

2Okondedwa,tsopanondifeanaaMulungu,ndipo sichinaonekechimenetidzakhalapakutitidzamuwonaIye mongaali

3Ndipoyensewakukhalanachochiyembekezoichimwa Iyeadziyeretsayekha,mongaIyealiwoyera

4Aliyensewochitatchimoamaphwanyansolamulo, chifukwauchimondikuphwanyamalamulo.

5NdipomudziwakutiIyeadawonekerakudzachotsa machimoathu;ndipomwaIyemulibeuchimo.

6Yensewakukhalamwaiyesachimwa; 7Anaaang’ono,asakunyengenimunthualiyense; 8IyeameneachitatchimoaliwochokeramwaMdyerekezi; pakutimdierekeziamachimwakuyambirapachiyambi.

ChifukwachaichiMwanawaMulunguadawonekera,kuti akawonongentchitozamdierekezi

9YensewobadwamwaMulungusachitatchimo;chifukwa mbewuyakeikhalamwaiye:ndiposakhozakuchimwa, chifukwawabadwakuchokerakwaMulungu.

10MwaichiaonekeraanaaMulungu,ndianaa Mdyerekezi:yensewosachitachilungamosaliwochokera kwaMulungu,kapenaiyewosakondambalewake.

11Pakutiuwundiuthengamudaumvakuyambira pachiyambi,kutitikondanewinandimzake

12OsatimongaKaini,ameneadaliwochokeramwa woyipayo,namuphambalewakendipoanamuphaiye cifukwaninji?Chifukwantchitozakezaiyeyekhazinali zoipa,ndizambalewakezolungama.

13Musazizwe,abaleanga,ngatidzikolidainu

14Tikudziwakutitachokakuimfakupitakumoyo, chifukwatimakondaabale.Iyewosakondambalewake akhalamuimfa

15Aliyenseameneamadanandim’balewakendiwopha munthu.

16Umotizindikirachikondi,chifukwaiyeanaperekamoyo wakechifukwachaife:ndipoifetiyenerakuperekamoyo wathuchifukwachaabale.

17Komaiyeamenealindichumachadzikolapansi,naona mbalewakealiwosowa,ndikutsekerezachifundochake kwaiye,nangachikondichaMulunguchikhalamwaiye bwanji?

18Tianaanga,tisakondendimau,kapenandililime;koma m’ntchitondim’choonadi.

19Umotizindikirakutitiriachowonadi,ndipo tidzatsimikizamitimayathupamasopake

20Pakutingatimtimawathuutitsutsa,Mulunguali wamkulukuposamtimawathu,nazindikirazonse

21Okondedwa,ngatimtimawathusutitsutsa,tirinacho kulimbikamtimakwaMulungu.

22Ndipochirichonsetipempha,tilandirakwaIye, chifukwatisungamalamuloake,ndikuchitazinthu zomkondweretsapamasopake.

23Ndipoilindilamulolake,kutitikhulupiriredzinala MwanawakeYesuKhristu,ndikukondanawinandi mnzake,mongaanatilamuliraife

24Ndipoiyewakusungamalamuloakeakhalamwaiye, ndiiyemwaiyeNdipom'menemotizindikirakutiakhala mwaife,mwaMzimuumeneanatipatsaife.

MUTU4

1Okondedwa,musakhulupiriremzimuuliwonse,koma yesanimizimungatiichokerakwaMulungu:chifukwa anenerionyengaambiriadatulukakulowam'dzikolapansi

2MwaichimuzindikiraMzimuwaMulungu:mzimu uliwonseumeneuvomerezakutiYesuKhristuanadza m’thupindiwochokerakwaMulungu

3NdipomzimuuliwonseumenesuvomerezakutiYesu Khristuanadzam’thupi,suchokerakwaMulungu:ndipo uwundimzimuwawokanaKhristu,umenemunaumva kutiukudza;ndipongakhaletsopanoulikalem’dziko lapansi.

4Tianainu,ndinuaMulungu,ndipomwawalakaiwo, chifukwaiyeamenealimwainualiwamkulukuposaiye wakukhalam’dziko.

5Iwoaliadzikolapansi,chifukwachakeamalankhulaza dzikolapansi,ndipodzikolapansilikumvaiwo

6IfendifeaMulungu:wodziwaMulunguamatimvera;iye wosachokerakwaMulungusatimveraifeM’menemo tizindikiramzimuwachowonadi,ndimzimuwa kusokeretsedwa

7Okondedwa,tikondanewinandimnzake:pakutichikondi chichokerakwaMulungu;ndipoyenseameneakonda, abadwakuchokerakwaMulungu,nazindikiraMulungu

8IyewosakondasadziwaMulungu;pakutiMulungundiye chikondi.

9UmochidawonekerachikondichaMulungukwaife,kuti MulunguanatumizaMwanawakewobadwayekhakudziko lapansi,kutitikhalendimoyomwaIye.

10Umomulichikondi,sikutiifetinakondaMulungu, komakutiIyeanatikondaife,ndipoanatumaMwanawake akhalechiombolochifukwachamachimoathu.

11Okondedwa,ngatiMulunguanatikondaifekotero, ifensotiyenerakukondanawinandimnzake

12PalibemunthuadawonapoMulungu.Ngatitikondana winandimzake,Mulunguakhalamwaife,ndichikondi chakechikhalachangwiromwaife

13M’menemotizindikirakutitikhalamwaIye,ndiIye mwaife,chifukwaanatipatsamzimuwake

14Ndipoifetawona,ndipotichitaumbonikutiAtate adatumaMwanaakhaleMpulumutsiwadzikolapansi.

15IyeameneadzabvomerezakutiYesualiMwanawa Mulungu,Mulunguakhalamwaiye,ndiiyemwaMulungu 16Ifetadziwandipotakhulupirirachikondichimene MulungualinachokwaifeMulungundiyechikondi; ndipoiyeameneakhalam’chikondiakhalamwaMulungu, ndiMulunguamakhalamwaiye.

17M’menemochikondichikhalachangwiro,kutitikhale olimbikamtimam’tsikulachiweruzo;

18Mulibemantham’chikondi;komachikondichangwiro chitayakunjamantha:chifukwamanthaalinachochizunzo Woopasakhalawangwirom'chikondi

19IfetimakondaIye,chifukwaanayambaIyekutikonda. 20Ngatimunthuanenakuti,NdikondaMulungu,nadana ndimbalewake,aliwabodza;

21NdipolamuloilitilinalolochokerakwaIye,kutiiye ameneakondaMulunguakondensombalewake

MUTU5

1YensewokhulupirirakutiYesundiyeKhristu,wabadwa kuchokerakwaMulungu;

2MwaichitizindikirakutitikondaanaaMulungu,pamene tikondaMulungu,ndikusungamalamuloake.

3PakutiichindichikondichaMulungu,kutitisunge malamuloake:ndipomalamuloakesaliolemetsa

4PakutichilichonsechobadwamwaMulunguchililaka dzikolapansi:ndipoichindichigonjetsochimenechililaka dzikolapansi,ndichochikhulupirirochathu

5Ndaniiyeameneagonjetsadzikolapansi,komaiye ameneakhulupirirakutiYesualiMwanawaMulungu?

6Uyundiyeameneadadzandimadzindimwazi,ndiye YesuKhristu;osatindimadziokha,komandimadzindi mwazi.NdipoMzimundiyewochitaumboni,chifukwa Mzimundiyechowonadi

7PakutipaliatatuameneamachitiraumboniKumwamba, Atate,Mawu,ndiMzimuWoyera:ndipoatatuawaali mmodzi

8Ndipoalipoatatuakuchitiraumbonipadzikolapansi, Mzimu,ndimadzi,ndimwazi:ndipoatatuawa avomerezanam’modzi

9Ngatitilandiraumboniwaanthu,umboniwaMulungu ndiwaukulu,pakutiuwundiumboniwaMulunguumene anachitiraumbonizaMwanawake

10IyeameneakhulupiriraMwanawaMulungualinawo umbonimwaiyeyekha;chifukwasadakhulupiriraumboni umeneMulunguadauperekawaMwanawake

11Ndipouwundiumboni,kutiMulunguanatipatsaife moyowosatha,ndipomoyoumenewuulimwaMwana wake

12IyeamenealindiMwanaalinawomoyo;ndipoiye amenealibeMwanawaMulungualibemoyo

13Zinthuizindakulemberaniinu,akukhulupiriradzinala MwanawaMulungu;kutimudziwekutimulinawomoyo wosatha,ndikutimukhulupirirepadzinalaMwanawa Mulungu

14NdipoichindichidalirochimenetilinachomwaIye, kutingatitipemphakanthumongamwachifunirochake, amatimvera;

15Ndipongatitidziwakutiamatimveram’chilichonse chimenetipempha,tidziwakutitirinazozopemphazimene tidazipemphakwaIye

16Ngatiwinaawonam’balewakeakuchimwatchimo losatilakuimfa,apemphere,ndipoiyeadzam’patsamoyo chifukwachaiwoameneamachimwaosatikuimfaPali tchimolakuimfa:sindikunenakutialipempherereilo.

17Chisalungamochonsendiuchimo:ndipopalitchimo losatilakuimfa

18TidziwakutiyensewobadwamwaMulungusachimwa; komaiyewobadwamwaMulunguadzisunga,ndipo woipayosamkhudzaiye

19NdipotidziwakutindifeaMulungu,ndipodzikolonse lapansiligonamwawoipayo

20NdipotidziwakutiMwanawaMulunguwafika, natipatsaifechidziwitso,kutitizindikireWoonayo,ndipo tirimwaWoonayo,mwaMwanawakeYesuKristuUyu ndiyeMulunguwoona,ndimoyowosatha.

21Tiana,pewanimafanoAmene

Turn static files into dynamic content formats.

Create a flipbook
Issuu converts static files into: digital portfolios, online yearbooks, online catalogs, digital photo albums and more. Sign up and create your flipbook.